Text
stringlengths 292
6.6k
| labels
int64 0
19
|
---|---|
Red Cross igawa magombeza 6, 720 Bungwe la zachifundo la Malawi Red Cross Society (MRCS) layambapo ntchito yogawira Amalawi ovutika, ana amasiye ndi okalambammaboma 14 a mdziko muno.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Ntchitoyi idayamba sabata yatha mboma la Mangochi komwe anthu 480 adalandira zofundazi, zomwe zidachokera kubungwe lina lotchedwa Japanese Blankets for Africa Campaign la ku Japan ndipo zadya ndalama zokwana K40 miliyoni.
Wachiwiri kwa wamkulu wa bungweli, Lizzie Mwambazi, aduza Tamvani kuti chaka chilichonse bungweli limagawa magombezawa nyengo yozizira ikafika pofuna kuthandiza anthu ovutika.
Takwanitsa zaka 20 tsopano tikugwira ntchito imeneyi ndipo tagawapo magombeza okwana 250 000 kwa ana amasiye, anthu okalamba ndi ovutikitsitsa. Chaka chino talandira magombeza 6 720 omwe tigawe mmaboma 14, kutanthauza kuti boma lililonse anthu 480 ndiwo achite mwayi, adatero Mwambazi.
Iye adati bungwe lawo limapereka thandizo losiyanasiyana kwa anthu potengera nyengo ndi zomwe zikusowa kwambiri panthawiyo ndipo adaona kuti nyengo yozizira anthu ambiri ovutika amakongwa.
Woyendetsa ntchito za kuofesi ya DC mboma la Mangochi, Bissaih Mtayamanja, adapempha anthu omwe adalandira nawo magombezawo kuti asagulitse koma akagwiritse ntchito yake podzitchinjiriza kumphepo.
Iye adapempha anthu omwe sadalandire nawo magombezawo kuti asadandaule chifukwa thandizo ngati limeneli lochokera kumabungwe limafika pangonopangono kuti anthunso azilandira pangonopangono.
Tikudziwa kuti anthu ofunika kulandira thandizo ngati limeneli alipo ambiri koma ochepa okha ndiwo achite mwayi lero ndipo kukadzabwera thandizo lina, enanso adzalandirako, choncho osachitirana nkhanza kapena nsanje, ayi, adatero Mtayamanja.
Iye adapemphanso anthu akufuna kwabwino omwe ali ndi kangachepe kuti atengerepo mtima womwe amaonetsa anthu a ku Japan poperekako kangachepeko kuti anzawo ovutika azipezako thandizo.
Gulupu Mapira, yemwe mwambo wogawa magombezawo udachitikira mdera lake, adati nzomvetsa chisoni kuti mabungwe akufuna kwabwino akamabwera ndi thandizo, anthu omwe amapatsidwa udindo wosankha anthu kapena kugawa amachita chinyengo.
Iye adapempha anthu mmaboma ena momwe katunduyu akupita kuti aonetsetse kuti anthu ovutika zenizeni ndiwo akulembedwa pamndandanda wa anthu olandira nawo, osati abale kapena anzawo.
Kulandira thandizo ngati ili sikoyamba koma zimadandaulitsa kuti anthu omwe amayeneradi kulandira nawo akubwerera kwawo manja ali mkhosi ndipo mchitidwe umenewu umachitika ngakhale pogawa chakudya kapena zipangizo zaulimi ndi ziwiya za mnyumba kwa anthu omwe akhudzidwa ndi ngozi zadzidzidzi, adatero Mapira.
Iye adapempha mwapadera kuti mabungwe asaiwale kukhazikitsa ntchito yogawa chakudya chifukwa madera ambiri anthu sakolola mokwanira kaamba ka momwe mvula idagwera chaka chino.
| 15 |
Akhalenso ndi moyo wautali Tsiku limenelo ndidakwiya zedi pa Wenela. Mkwiyo wanga udali waukulu zedi moti ndidafuna kuphulika. Inde, udali mkwiyo waukulu zedi moti kuchita chibwana nzimbe ndithu ikadamera pamsana! Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Mminibasi imene ndinkaitanira nthawi imeneyo munkalira nyimbo ya King Yellowman, inde, mmodzi mwa oimba chamba cha dancehall kuchokera ku Jamaica. Mutu wa nyimboyo ndi Zungguzungguguzungguzeng. Amene sakuidziwa nyimbo imeneyi ngoyenera kudzidabwa chifukwa inetu ngakhale ndili kwathu kwa Kanduku, mawu ake ndinkawadziwa bwino: Zungguzungguguzungguzeng Zungguzungguguzungguzeng Seh if yuh have a paper, yuh must have a pen And if yuh have a start, yuh must have a end Seh five plus five, it equal to ten And if yuh have goat, yuh put dem in a pen And if yuh have a rooster, yuh must have a hen, now: Chidandikwiyitsa kwambiri chidali chakuti mminibasimo mudatsika munthu wachialubino. Mzibambo adabopha ulusi mochititsa kaso. Atatsika munthuyo, anthu adayamba kuliza malikhweru. Ena adali kukuwa: Mamiliyoni awo!!! Mawu amenewa ndiwo adandikwiyitsa zedi. Ndidagwira mmodzi mwa anthu amakuwawo. Ndidamulawitsa makofi.
Kupusa! Amene mukukuwa zopusazi ndinu oipa, chimodzimodzi amene amapha maalubino ati kuti akachite zizimba. Kulemera kwake kuti? Ndipo chuma chake chodyedwa ndi njenjete chomwechi? ndidafunsa mozaza.
Nditapita kumalo aja timakonda, ndidapeza akuvina nyimbo ya Kenneth Ninganga ndi Geoffrey Zigoma. Koma kudali dansi yotha malo. Ndipo mawu anthetemya a Zigoma adanditenga mtima osakhala masewera.
Mayo mayo, mayo mayo ndathera pano! Takondwera mwalowa mbanja aye.
Itatha nyimboyo, wapamalopo, Gervazzio, adatsegula wailesi kuti timvere nkhani.
Mwina nkumva kuti Moya Pete wanenapo chiyani za kubedwa, kuphedwa ndi kunyozedwa kwa maalubino, adatero.
Woweruza milandu wina walamula kuti munthu amene anaba munthu wachialubino wina akaseweze kundende zaka ziwiri, adali kutero wowerenga nkhani.
Abiti Patuma adakwiya. Mtima wake umachita kumveka kugunda ngati uphulika! Zaka ziwiri basi? Munthuyo amafuna akagulitse munthu wachialubinoyo kuti achotse ziwalo zina ati zizimba ndiye kungomupatsa zaka ziwiri kundende? Munthu wakuba ngombe akupatsidwa zaka 7 koma wakuba munthu mnzake kungopatsidwa zaka ziwiri basi? adazaza.
Nanenso mkwiyo udachititsa mwazi wanga kuthamanga.
Zilango amati zizichititsa ena kuti asayerekeze kupalamula. Chilango ngati ichi chingaopseze ena? Enatu akufukula mitembo ya maalubino ati zizimba. Ayi ndithu, ufiti wotere wafika povuta, ndidatero.
Mkwiyo wandizinga. Mtima wanga ukupweteka. Ndikumva kutentha ngati munthu wodya nsima yamoto, ndiwo zake khwanya wothiridwa tsabola wakambuzi wochuluka komanso atakhala padzuwa la 12 koloko masana.
Mmutu mwanga mudayamba kuyenda nyimbo ya Salif Keita. Ngati mu Africa muli anthu odziwa kuimba, Salif Keita ndi mmodzi mwa iwo. Ngakhale ndi wachialubino, Salif ali ndi luso ndipo amadziwika padziko lonse lapansi chifukwa cha nyimbo zake zogwira mtima. Ndimukumbuka bwino chifukwa tsiku lomwe adabwera ku Malawi ndidanyamula zikwama ndi magitala ake kulowera ku French Cultural Centre.
Nyimbo yake idali ya Folon, imene adaimba ndi wotchuka winanso, Youssour Ndor.
Koma abale nkhanza izi ziyenera kutha. Momwe ndikuonera mchitidwe wonyansawu udayamba kalekale. Ndikumbuka kalekale tinkauzidwa kuti ma alubino amangosowa, samwalira. Ndiye kuti nkhanzazi zidayamba kale. Anthu akuba anzawowa adayamba izi kalekale, adatero Abiti Patuma.
| 15 |
Papa Wayamikira Asodzi, Ogwira Ntchito Pa Madzi Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Francisco wayamikira anthu ogwira ntchito pa madzi komanso asodzi chifukwa cha ntchito yawo yothandiza kudyetsa anthu.
Malinga ndi malipoti a Vatican Radio, Papa walankhula izi lachitatu kudzera mu uthenga wake wa pa kanema wopita ku utumiki wa mu Mpingo wa Katolika womwe umaona ntchito za pa madzi.
Kudzera mu uthengawo Papa Francisco wayamikira anthuwa chifukwa chodzipereka ngakhale pano kaamba ka mliri wa Coronavirus akukumana ndi zovuta zambiri.
Iye wati ngakhale kuti ntchitoyi ili ndi zovuta zake komabe anthuwa amayetsetsa kubweretsa chakudya kwa anthu ambiri omwe amakonda ndiwo ngati nsomba ndi zina zambiri zopezeka mmadzi.
Papa Francisco wati mliri wa Coronavirus wachititsa kuti anthuwa azikhala pa madzi nthawi yaitali asadakumane ndi mabanja awo komanso abwenzi poopa kupatsirana nthendayi.
Malinga ndi nthambi ya bungwe la United Nations yomwe imaona za anthu ogwira ntchito International Labour Organisation yati anthu oposa 150,000 akakamizidwa kukhala pa madzi osakumana ndi mabanja awo komanso abwenzi kaamba ka mliri wa Coronavirus.
Papa Francisco watsimikizira onse ogwira ntchito za pa madzi za mapemphero ake ndipo wakumbutsanso anthuwa azinyadira ntchito yao popeza ophunzira oyambirira a Yesu Khristu adali asodzi.
Pomaliza sadaiwale kulimbikitsa onse omwe amaona za moyo wa uzimu wa anthu ogwira ntchito za pa madziwa.
Utumiki wa mu Mpingo wa Katolika womwe umaona ntchito za pa madzi (Apostleship of the Sea) nkhoswe yake ndi Amayi Maria Our Lady Star of the Sea.
| 14 |
MEC Ilowa Pansika By Slyvester Kasitomu Bungwe lowona za chisankho mdziko muno la Malawi Electoral Commission (MEC) lalengeza likhala likugulitsa wina mwa katundu wa bungweli yemwe wakhala asakugwira ntchito kwa nthawi yaitali.
Bungweli lalengeza izi kudzera mu chikalata chomwe latulutsa. Mneneri wa bungwe-li Sangwani Mwafuliwa wati a Malawi asakhale ndi nkhawa yoti katundu yemwe akugulitsayu ndi yemwe angwiritsidwa ntchito pa chisankho chomwe chinachitika mdziko muno mwezi watha ponena.
Mwafulirwa: Tatsata dongosolo loyenera Katundu yemwe tikugulitsayu ndi yekhayo yemwe samagwira ntchito komanso anagwiritsidwa ntchito mu zisankho zomwe zinachitika mdziko muno zaka zapitazi, anatero a Mwafulirwa.
Mwazina iwo ati pogulitsa katunduyi atsata njira zoyenera zakagulitsidwe ka katundu wa boma.
A Mwafulirwa anati, Kuti tigulitse katunduyi tatsata dongosolo loyenera ndipo tiwatsimikizire a Malawi onse kuti tikudziwa za chigamulo cha khothi ndipo ife a bungwe la MEC timalemekeza malamulo a dziko lino choncho pa katundu amene akugulitsidwayu palibe amene akukhudzidwa ndi milandu yomwe ili kukhothi kapena anthandiizira pa ntchito yokonzera chisankho cha pa 21 May.
A Mwafulirwa amemeza mabungwe omwe si aboma komanso atsogoleri a zipani zosiyanasiyana mdziko muno kuti adzafike pa tsiku la malondali kuti adzaone katundu yemwe akugulitsidwayu.
Bungwe loyendetsa chisankho mdziko muno ati lakonza zogulitsa katunduyi yemwe sakugwira ntchito ndipo amangowonongeka ku malo osungira katundu wa bungweli.
| 11 |
Pewani ngozi, kuberedwa Nyengo ya Khirisimasi ndi Nyuwere kumachuluka ngozi za pamsewu, mchitidwe wa umbava ndi umbanda komanso ngozi zina monga kumira mmadzi akusangalala.
Nthambi yoona za ngozi za pamsewu ya Directorate of Road Traffic and Safety Services (DRTSS) yakhala ikupereka malangizo kudzera mnyuzipepala kuyambira pa December 14 2016 pofuna kuti anthu adziwe msanga za kapewedwe ka ngozi zisangalalo zisadafike pachimake.
Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Ngozi iyi idachitika sabata yangothayi Nthambiyi yati kupatula zopangitsa ngozi zina, nkhani yaikulu imakhala kuyendetsa galimoto chiledzerere kapena galimoto zosayenera kuyenda pamsewu zomwe zimaononga miyoyo ndi katundu.
Chikalatacho chidatinso oyendetsa galimoto akuyenera kupereka mpata odutsa kwa anthu mmalo monse mowolokera ndipo asayankhule palamya akuyendetsa galimoto poopa kuti chidwi chawo chingathawire ku lamyako mmalo moyendetsa galimoto.
Nthambiyo idatinso okwera ali ndi udindo odziteteza popewa kukwera galimoto zomwe zadzadza kwambiri ndi kupewa kukakamiza oyendetsa kuti azithamanga ngati achedwa paulendo wawo.
Nawo apolisi ati anthu ali ndi udindo woteteza miyoyo ndi katundu wawo potsatira ndondomeko zomwe iwo amapereka chaka ndi chaka monga kuonetsetsa kuti asiya munthu okhwima maganizo pakhomo akamachoka.
Mneneri wa polisi James Kadadzera adati nthawi zambiri chifukwa chokomedwa, anthu amasiya pakhomo palibe aliyense nkupita kokasangalala ndipo pobwera amapeza nyumba yathyoledwa.
Njira ina nkuonetsetsa kuti pomwe ana akusewera kapena kusangalala, pali munthu wamkulu owayanganira kuopa kuti angabedwe kapena kuvulala ngati ali okhaokha, adatero Kadadzera.
| 10 |
Kasambara: Akhazikitsa chimbale mwezi uno Martha Kasambala ndi woimba nyimbo zauzimu ndipo amakhala ku Mzuzu. Iye ali ndi zimbale ziwiri ndipo mu December muno akuti akhazikitsa chimbale chake chatsopano chotchedwa Amasamala. Mtolankhani wathu DAILES BANDA adacheza naye motere: Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Ali ndi uthenga wapadera mchimbale chatsopano: Kasambara Tikudziweni Ndine Martha Kasambara wa mmudzi mwa Malanda ku Chintheche mboma la Nkhata Bay. Ndili pabanja ndipo ndili ndi mwana mmodzi.
Mbiri yako pamaphunziro njotani? Ndidaphunzira pulaimale yanga pa Lilongwe LEA pomwe ndidalemba mayeso anga a Standade 8; sekondale ndidaphunzira ku Chipasula ku Lilongwe komweko. Ndidakapanga maphunziro a zauphunzitsi ku Tanzania komwe ndidaphunzitsa mwakanthawi pangono ndipo pakadalipano ndikupanga bizinesi.
Ndiye zoimbaimbazi mudayamba bwanji? Ndidayamba kuimba ndili wachichepere kwambiri koma chimbale changa choyamba ndidatulutsa muchaka cha 2008 chomwe chimatchedwa kuti Zonse ndi Yesu. Chimbale chachiwiri Nganganga ndi Yesu chidatuluka mu 2010. Chimbale chatsopano chotchedwa Amasamala ndichikhazikitsa mu December muno.
Uthenga waukulu womwe wanyamula ndi wotani mchimbalechi? Kwakukulu uthenga omwe uli mchimbalechi ndi wachilimbikitso kwa Akhristu anzanga munyengo zili zonse zomwe iwo akudutsamo. Yesu amasamala anthu ake ndipo tikamudalira iye sitidzakhumudwa chifukwa chisomo chake ndi chokwanira.
Kodi mfundo za munyimbo zimenezi mumazitenga kuti? Nyimbo zanga kwambiri zimachokera pa maulaliki a kutchalitchi komanso ndikamawerenga Baibulo ngakhalenso nthawi zina zinthu zomwe ndikuona ndi kukumana nazo.
Ndi zinthu ziti zomwe mungakonde kuti zisinthe kumbali ya zoimba mMalawi muno? Mmastudio mwathu mukufunika zipangizo zamphamvu zojambulira nyimbo ngati mmene kulili kumaiko a anzathu, monga ku South Africa, chifukwa nyimbo zimamveka bwino kwambiri.
Phindu mukulipezamo mukuimbaku koma? Mmbuyomu zinthu zimavuta koma pakalipano ndi chimbale chatsopanochi, tsogolo lopindula likuoneka.
| 9 |
Mtembo usagone panoAchipatala Pasathe tsiku mtengo wanu musadadzatenge. Uthenga omwe a zipatala za Rumphi ndi Machinga akuuza anthu chifukwa cha kuonongeka kwa malo wosungira mitembo pachipatalapo.
Pachipatala cha boma ku Rumphi, zaka ziwiri zatha malo osungira mitembowa atasiya kugwira ntchito pamene ku Machinga, miyezi itatu yatha malowa atasiya kugwira ntchito.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Jobe: Boma lichitepo kanthu Izi sizidakomere anthu amene amagwiritsa ntchito zipatalazi amene anena kuti boma ndi mabungwe alowererepo kuti zotere zisinthe.
T/A Nyambi ya mboma la Machinga akuti pakhala povuta kuti anthu azikatenga thupi la malemu tsiku lomwelo chifukwa palibe amene amakonzekera maliro.
Ambiri tikukhala kutali ndi chipatalachi. Zovuta zikagwa timadalira kuti pathe tsiku kuti tipeze mayendedwe. Tikuvutika chifukwa kuchipatalako kulibe galimoto zokwanira kuti azikatisiyira zovuta pakhomo pathu, adatero Nyambi.
Mneneri wa chipatala cha Machinga, Clifton Ngozo akuti sangachitire mwina chifukwa ngati angasunge thupi kwa nthawi ndiye kuti lingathe kuonongeka.
Kudachitika ngozi, tidasunga matupi amene amakha magazi. Padatha masiku awiri kuti matupiwo apite kukaikidwa koma kudali fungo loipa. Ndiye sizithekanso kuti tisunge mtembo pokhapokha malowa atakonzedwa, adatero Ngozo.
Iye adati ngati atapitirira kumagoneka mitembo ndiye kuti zingabweretse zotsatira zoipa monga matenda kwa amene akugwira ntchito kumalowa.
Poyamba timasunga mitembo kwa masiku oposa awiri kapena atatu koma akamadzatenga mtembowo umakhala uli bwinobwino. Panopa sizingathekenso chifukwa malowa aonongeka.
Panopa uthenga omwe tikuuza anthu amene amagwiritsa ntchito malowa ndikuti sitikwanitsanso kuti matupi azigona kumeneku. Zovuta zikachitika atha kusunga koma asagone chifukwa aonongeka, adatero Ngozo.
Kuchipatala cha Rumphi, anthu adasiya kugoneka mitembo chifukwa cha kuonongeka kwa malo osungira mitembo.
Mneneri wa chipatalachi Bwanalori Mwamlima akuti malo osungira mitembo adaonongeka zaka khumi zapitazo koma akhala akukonzetsa mpaka 2015.
Panopa sitingakonzenso, chifukwa pena tikakonza sichimachedwanso kuonongeka. Apapa zavuta ndipo tasiya kugoneka mitembo chifukwa ikumaonongeka, adatero Mwamlima.
Iye akuti vuto nkuti zipangizozi zakhalitsa. Ndikakumbuka bwino, zipangizozi zidaikidwa mma 1976, zakhala zikugwira ntchito mpaka lero, adatero Mwamlima.
Izi zakhumudwitsanso mkulu wa bungwe loona za umoyo la Malawi Health Equity Network (Mhen) George Jobe amene wati aphungu a Nyumba ya Malamulo akuyenera aikambirane pamene akhale akukumana.
Amene adamanga nyumba yachisoni adali ndi cholinga ndipo adaona kufunikira kwake. Izi si zoona kuti mpaka malowa asiye kugwira ntchito chifukwa talephera kuwakonza.
Palibe amene amayembekezera maliro pamene wapita kuchipatala. Ndiye simunganene kuti maliro akangochitika basi munyamule, adatero Jobe.
Ku Salima nakonso akhala akukumana ndi mavuto omwewa koma pano zidayenda pamene malo osungira mitembowo adakonzedwa.
T/A Mwanza wa mbomali akufotokoza. Tidakumana ndi mavutowa koma panopa zinthu zilibwino pachipatalachi chifukwa adakonza, adatero Mwanza.
| 15 |
Idali nyengo ya pasaka Wina adapitira ntchito yokatola zochitika pa tchuthi chokumbukira mazunzo ndi kuuka kwa Ambuye Yesu pomwe wina adapita kukapuma monga tchuthi koma mapeto ake idasanduka nyengo yoti awiriwa awone zomwe Mulungu adawakonzera.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Mayamiko Seyani, yemwe panthawiyo amagwira ntchito ya utolankhani kukampani ya Nation Publications Limited (NPL) adali kalikiliki kutola zochitika zosiyanasiyana pomwe maso ake adakagwera pa Nicra Chikopa yemwe amadikira abale ake kuti akalowe mmadzi akasambire.
Mayamiko akuti atangomuona Nicra, ntchito yonse idasokonezeka ndipo sadaupeze mtima mpaka adatsatira pomwe padali namwaliyo nkuyamba kucheza naye.
Mayamiko ndi Nicra tsiku la chinkhoswe chawo Ndidali ndi anzanga pa nthawiyo koma ndidawasiya ndipo nawonso adandimvetsetsa chifukwa sinkadachitira mwina ayi koma kusendera kufupi, adatero Mayamiko.
Nicra akuti machezedwe a Mayamiko adamusangalatsa kwambiri moti adaiwala zokasambira abale ake omwe amadikira atafika.
Tidacheza ngati anthu oti tidadziwana kalekale pomwe ayi ndithu kadali koyamba moti adandipatsa chidwi kwambiri, adatero Nicra.
Chitatha tchuthi, awiriwa akuti adakumananso mumzinda wa Blantyre momwe onse amakhala ndipo macheza awo adapita patsogolo kufikira pomwe Mayamiko adamasuka lilime nkufunsira.
Zonsezi akuti zinkachitika mchaka cha 2014 ndipo kuyambira apo mpaka lero, chibwenzi chawo chakhala chikuyenda bwino moti pa 4 October chaka chomwe chino adamanga chinkhoswe kuyembekeza ukwati oyera chaka chamawachi.
Mayamiko akuti kwa iye Nicra ndi mkazi yekhayo yemwe adamutenga mtima mpaka njala ya chakudya kutha ndipo akuti salotako zoti nkudzalekana naye.
Nicra naye akuti chake nchisangalalo chokhachokha popeza mwamuna wa kukhosi kwake ndipo naye akuti alibenso nkhawa za tsogolo lowala.
Palibe yemwe amada nkhawa atapeza chinthu chomwe amalakalaka mmoyo mwake. Ine ndidapeza mwamuna yemwe ndinkalakalaka wachikondi, wachilimbikitso komanso owopa Mulungu, adatero Nicra.
Mayamiko amachoketra mmudzi mwa Nankwana kwa T/A Makwangwala mboma la Ntcheu pomwe Nicra amachokera mmudzi mwa Nguluwe, T/A Bvumbwe, Thyolo.
| 15 |
DPP Yati Siyigonja Pochita Zionetsero Chipani cha Democratic Progressive (DPP) lachitatu chinachita ziwonetsero chigawo chaku mmawa kwa dziko lino ati posakondwa ndi momwe bwalo la zamalamulo la Constitutional Court lidagamulira mulandu wa za chisankho cha president.
Ziwonetserozi zinachitikira mu mzinda wa Zomba ndipo zinayambira ku Chinamwali mpaka kukafika ku khonsolo ya bomalo, komwe adakapereka chikalata chamadandaulo awo kwa mkulu wa mzinda wa Zomba a Charles Thombozi, komanso kwa bwanamkubwa wa bomalo Dr. Raphael Piringu.
Otsatira chipani cha DPP pa zimodzi mwa zionetsero zomwe anachita Chipani cha DPP chati chikufuna kuti bungwe la Anti Corruption Bureau (ACB) lifufuze ma Judge omwe amamva mulandu-wu popeza akuwaganizira kuti adalandira ziphuphu kuti agamule mokomera Dr. Saulos Chilima komanso Dr. Lazarus Chakwera.
Chikalatachi chikutinso mmodzi mwama Judge omwe amamva mlanduwu Dingiswayo Madise ndi mbale wake wa Dr. Saulos Chilima choncho samayenera kuzenga nawo mulanduwu.
Polankhulanso kwa atolankhani mlangizi wa president pa nkhani zandale a Francis Mphepo wati oweluza mulandu-wu zimene anachita ndi zopanda chilungamo.
Khothi la zamalamulo linanena kuti ifeyo a DPP sitinabele kusonyeza kuti siife olakwa anachita izi ndi a MEC ndiyeno ngati ife sitinabele ndi chifukwa chiyani alamula kuti chisankhochi chichitikenso kumeneko ndiye kupanda chilungamoko, anatero a Mphepo.
Zimenezi ndi ziwonetsero zachiwiri kuchitika kutsatira zoyamba zomwe zinachitika lolemba mu mzinda wa Blantyre ndipo pali chikonzero chakuti ziwonetsero za mtunduwu zichitikanso ku Lilongwe komanso ku Mzuzu msabatayi.
| 11 |
Atumiki ndi Ofunika Palimbana ndi COVID-19 Ngoma Ansembe ndi asisiteri a mu dayosizi ya Chikwawa awatsimikizira kuti ndi ofunikira kwambiri pa ntchito yolimbana ndi kufala kwa mliri wa COVID-19 omwe ukuyamba ndi kachirombo ka Coronavirus.
Mlembi wamkulu mu ofesi ya nthambi ya zaumoyo mu dayosiziyi a Louis Ngoma anena izi lolemba ku Chikwawa Cathedral pa maphunziro omwe unduna wa zaumoyo kudzera pa chipatala cha boma la Chikwawa, anakonzera atumikiwa.
A Ngoma anati atumikiwa ali pa ntchito yayikulu yofalitsa uthenga kwa akhristu awo pa kapewedwe koyenera ka matenda a COVID-19. Polankhulanso ku mwambowu, bambo Matthews Semba, omwe amayanganira nthambi ya zaumoyo mu dayosiziyi ayamikira a za umoyo pofika ndi maphunzirowa kwa atumuki a mpingo mu dayosiziyi.
Pambuyo pa maphunzirowa nthambi ya zaumoyo mu mpingowu mu dayosiziyi inaperekanso zipangizo zodzitetezera ku kachilombo ka Coronavirus kwa ansembe ndi asisiteri ndipo zonse ndi za ndalama zokwana 1 Million Kwacha.
| 6 |
Amayi Amachawi Akufuna Chilungamo Chiwoneke pa Kuphedwa Kwa Mzimayi ku Mangochi Gulu la Amayi A Machawi mboma la Mangochi lati lifunitsitsa kuti pakhale chilungamo pa mlandu wa kuphedwa kwa mzimai wina wachikulire wa mbomali yemwe amaganiziridwa pa nkhani ya ufiti.
Wapampando wa gululi mai Triza Masauli ndi omwe alankhula izi lachisanu mbomali pa msonkhano wa atolankhani.
Iwo ati ndi ufulu wa munthu aliyense kukhala ndi moyo, choncho pakuyenera kuti pakhale dongosolo labwino loyendetsera mlanduwu ndi cholinga chakuti chilungamo chisaponderezedwe.
Ndife okhudzidwa kwambiri chifukwa cha imfa ya mayi mzathu yemwe anangophedwa ngati nkhuku. Timati tipemphe kuti zimenezi zisadzachitikenso kuno ku Mangochi, anatero a Masauli.
Pamenepa iwo apempha achitetezo komanso magulu owona za maufulu a anthu kuti atenge gawo lalikulu pa kafukufuku wa nkhani-yi.
| 7 |
Basi ayisempha Tsiku limenelo sitidakhale pa Wenela. Palibe ojiya, osolola, osenza ndi oitanira amene adatsala pa Wenela.
Tidakwera galimoto la mkulu wina kulowera ku Lilongwe. Si kuti timapita kuja kulikulu la boma kumene masamu ogula mmera asokonekera.
Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Sindingakambe nkhani imeneyo chifukwa tonse tikudziwa kuti lingaliro la Dizilo Petulo Palibe, malinga ndi kufotokoza kwa Joloji Chiponda, lidali logula chimangacho ku Brazil. Zoona mpaka kuoda chimanga ku Brazil! Nkhani ya chimangayi kwa ine ndiyongotaya nthawi. Ngati Moya Pete adalamula asilikali ake kukwidzinga uja wogina ndi amayi oposa 100 bwanji akulephera kulamulanso amene akuganiziridwa kukazinga mmera wa tonse pano pa Wenela? Zosamveka konse kuti mzimayi woti akufuna kugula chimanga choti adye pakhomo pake, mmalo mopita yekha kumsikako kutuma wina kuti akamugulire kenako nkumadandaula kuti waberedwa! Abale anzanga, tingoyerekeza kuti mwalemba wantchito, ndiye mukumukaikira kuti anaba ndiwo. Kenako mukuuza akazi kapena amuna anu kuti afufuze momwe anabera ndiwozo, wantchito wanu akapita pachulu nkumakuwa kuti: Sindinabe ine! Sindinabe! Chomwe ndimadabwa pano pa Wenela nchakuti nchifukwa chiyani aliyense amafuna kutalika zala pankhani za chimanga? Tidamvapo kuti Adona Hilida adagulitsa matani ochuluka kupita nawo ku Kenya. Nanga za Thursday Jumbo uja naye adadyapo zake za chimanga. Za makuponi ndiye ndisachite kunena.
Nsataye nazo nthawi izo.
Chaka chino talowa Talowa ndi adani omwe Akufuna moyo wanga Kuti aononge Chauta thandizeni Iyi ndi nyimbo imene tinkamvera mugalimoto ya mkulu amene adatitenga. Tidafika kubwalo la mpira latsopano kumene zipolopolo ndi nyerere zimamenyana. Inu, munthu nkupha nyerere poyiwombera! Ndidangomva kuti ena adathyola mipando, kutenga makalilole ndi zina zotero! Komanso abambo ena ankalowa kuzimbudzi za akazi! Utatha mpira, sindikudziwa kuti udatha bwanji, Abiti Patuma adandikoka kuti timuthawe mkulu uja.
Tidakakwera basi imene sindikuyidziwa bwino. Mudali anyamata a Chimwemwe kwambiri. Iwo amangoti 5 kwa 1, 5 kwa 1. Onse atamuona Abiti Patuma adakuwira limodzi: Abiti Patuma! Yo-yo-yo! Wina adamukumbatira, wina kumupsopsona patsaya.
Osadanda, mwayiphula basi! Ndikuthangatani nonse mbasi momwe muno, adatero Abiti Patuma.
Koma abale! Kudalitu kulandirana! Basi imamveka ndithu kuti mashoko siali bwino komabe mmodzimmodzi adali kulandira chithandizo kuchokera kwa Abiti Patuma.
Adati tinyamuke, ulendo wobwerera pa Wenela.
Tili mnjira, yemwe amaoneka kuti ndi mkulu wa anyamatawo adati: Tikakafika ku Mwanza, tikadzera kwa Ayaya tikayamike chifukwa watithandiza kupeza basi.
Ulendo wa kwa Ayaya sunatheke chifukwa basi idatchona pa Manjawira. Poyamba tinkadya kanyenya kuti mwina iyenda. Kenako kudali kusaka mango, ngumbi ndi zina mpaka mdima udagwa.
| 1 |
Kusintha lamulo la ufiti kwachedwa udyo Kuchedwa kwa ntchito yosintha lamulo lokhudza zaufiti kukuchititsa kuti okalamba amene akuwaganizira kuti ndi mfiti apitirire kuzunzidwa komanso kuphedwa, atero a mabungwe ena.
Polankhula ndi Msangulutso padera-padera, mkulu wa bungwe limene limati kulibe ufiti la Association for Secular Humanism (ASH) George Thindwa komanso mkulu wa bungwe losamalira achikulire la Friends of the Elderly Mike Magelegele ati kuchedwa kwa ntchitoyi kukuchititsa kuti nkhanza kwa okaikiridwa ufiti zipitirire.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Akuchulukira ena akuzuzidwa mpaka kuphedwa chifukwa chowakaikira ufiti Nthambi yapadera younikira zosintha malamulo okhudza zaufiti ya Special Commission on Review of the Witchcraft Act yakhala ikumva maganizo a anthu pa zosintha malamulowo ndipo ikuyembekezeka kumaliza zonse mu July chaka chino. Ntchito yofufuzayi idayamba zaka 10 zapitazo.
Thindwa adati: Ntchitoyi ikuchedwa chifukwa cha ndondomeko yomwe bungwe lofufuzalo likutenga komanso akusowa thandizo. Mmalo molunjika pa zaufiti kuti athetse vuto, iwo afika mpaka kukambirana za chipembedzo cha satana.
Iye adati izi zili apo, nkhalamba zina zikuvutitsidwa komanso kuphedwa pachabe chifukwa palibe umboni wa ufiti.
Malinga ndi Thindwa, lamulo latsopano la ufiti likuyenera kulunjika poti aliyense wonena mnzake kuti mfiti aziyankha mlandu wothera kundende osapatsidwanso mpata wopereka chindapusa.
Ena amangowanamizira agogo kuti ndi mfiti kuti awalande minda, adatero Thindwa.
Magelegele adati bungwe lake lakhudzidwa chifukwa cha kuchedwa kwa ntchitoyi chifukwa ambiri ataya miyoyo yawo.
Tikupempha boma kuti tigwirane manja poyesetsa kuti zinthu zisinthe, adatero Magelegele.
Iye adatinso chiyambireni chaka chino paphedwa agogo 8, zomwe zikungoonetsa kuti ntchito ndiyaikulu.
Dziko lino likugwiritsa ntchito lamulo la chitsamunda lomwe lidakhazikitsidwa mu 1911 loti kulibe ufiti. Koma pomwe ntchitoyi ikuyenda pangonopangono ngati nkhono, agogo akupitirira kuvutika.
Komatu akadaulo pa malamulo, kaganizidwe komanso mafumu akukhulupilira kuti mchitidwewu ukhonza kuchepa ngati lamuloli lingakhazikitsidwe mwa changu.
Mmodzi mwa katswiri pa kaganizidwe pachipatala cha amisala cha St John of God ku Mzuzu, Ndumanene Sulungwe adati agogo ambiri amaphedwa chifukwa chodwala nthenda yoiwala, zimene zimachititsa kuti akamafunsidwa mafunso pamene akukaikiridwa ufiti amayankha zosemphana.
Iye adati ena mwa agogowa amaiwala ngakhale dzina la mudzi wawo kumene ndipo anthu akawapeza ali obalalika chomwecho, amati ndi mfiti ndi kuwachita chipongwe.
Choncho iye adapempha omwe akukonza lamulolo kuti ayesetse kuteteza agogowa.
Polankhulapo wachiwiri kwa mkulu woyendetsa ntchitoyi, Clotilda Sawasawa adavomereza kuti agogo, alubino ndi ana ndi amene ali pampani pa nkhani zokhudzana ndi kukayikiridwa ufiti.
Ndipo Sawasawa adavomerezanso kuti ntchitoyi yakhala isakuyenda mwachangu chifukwa chosowa ndalama.
Ndalama zoyendetsera ntchitoyi zakahala zikutivuta, choncho sizimayenda kwenikweni koma pano tiyesetsa kuthamangitsa zinthu kuti pofika mwezi wa July chaka chino tikhale titamaliza kutolera maganizo, adalongosola motero.
Ngati mmodzi mwa anthu okhudzidwa ndi nkhanizi, Chistopher Ndovi yemwe ndi wa chi alubino adauza Msangulutso kuti wakhala akuvutitsa kuchokera ali wachichepere.
Padali nthawi ina, mnzanga ankafuna nyama yochokera kumbuyo kwa khosi langali ndi tsitsi langa la pankhongo kuti akapangire mankhwala.
Zidafika povuta mpaka kumanditsatira kunyumba. Koma agogo anga ndiwo adanditeteza, adalongosola Ndovi.
Nayo Mfumu Mwenemsuku yochokera mboma la Chitipa idati ndi zoona kuti agogo ndi ana ndiwo akukhudzika kwambiri ndi zaufiti.
Iye adati ana ambiri akumaulula kuti agogo ndiwo akuwaphunzitsa ufiti ndipo pena agogowa amalephera kudzifotokoza pomwe nthawi zina amavomera ndithu.
| 19 |
Adutse ndani mu Standard Bank? Ndime ya kotafainolo mu Standard Bank Cup yafika podetsa nkhawa pamene matimu anayi akuyenera kutsanzikana ndi chikhochi sabata ino.
Pamene timalemba nkhaniyi dzulo nkuti matimu a Civo ndi Dedza Young Soccer akuswana pa Civo Stadium. Dedza itatulutsa Kamuzu Barracks kudzera mmapenote ulendo wapitawo, dzulo imayenera kuona ngati ulendo ukhale wopitirira kapena kuthera panjira.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Lero ndiye ulipo wankhodzo za pusi pa Kamuzu Stadium pamene Red Lions ithambitsane ndi Be Forward Wanderers.
Wanderers idatulutsa Mafco kudzeranso mmapenote. Lero kodi Wanderers ichita zakupsa? Anthu ambiri ali ndi chikaiko malinga ndi kugonja motsatizana kwa Wanderers muligi ya TNM, koma kochi Elijah Kananji akuti awa ndi masewero osiyana ndipo akuona timu yake ikuphulapo kanthu lero.
Anyamata akungofunika kuwalimbitsa mtima, koma ndilibe chikaiko malinga ndi momwe akumenyera kuti masewero ndi Red Lions titha kusangalala, adatero Kananji.
Nayo Red Lions ikukumana ndi Wanderers itakumana ndi masautso pamene adagonja ndi Big Bullets 4-2 mligi. Koma Collings Nkuna akuti akubwera pa Kamuzu kuchokera ku Zomba ndi cholinga chofuna kupambana.
Ija idali ligi, apa tikukamba za chikho. Tikuyembekeza kuti tichita bwino mmasewero amenewa, adatero Nkuna.
Mpira wina lero ali pakati pa Silver Strikers ndi Blue Eagles pa Silver Stadium. Matimu onsewa zawayendera kumathero a sabata imeneyi muligi, Silver itapuntha Dedza 2-1 pamene Eagles idawalira Civo 4-1.
Silver, kukhala timu yomwe ikusunga chikhochi, sidagonjepo mligi chibwerereni Young Chimodzi ngati kochi.
Mawa ndiye kukhale fumbi ku Civo pamene Moyale Barracks ikhale ikusambitsana ndi Bullets. Bullets ikungochoka kosemphana ndi chikho cha Carlsberg chomwe idachisiya mmanja mwa Wanderers.
| 16 |
Akagwira Ukayidi Kaamba Koba Phone, Laptop sizes="(max-width: 300px) 100vw, 300px" /> Bwalo loyamba la milandu mboma la Mangochi lalamula bambo wina kuti akakhale kundende ndikukagwira ntchito yakalavula gaga kwa zaka ziwiri ndi miyezi 6 atamupeza olakwa pa mulandu wothyola komanso kuba katundu mnyumba zina mbomali.
Bwaloli kudzera kwa wapolisi wotengera milandu kukhothi Augustus Kagwira linanva kuti mwamunayu Issa Mussa wa zaka 20 zakubadwa anathyola Zenera la nyumba ya a Mohamad Adam ndi kubamo lamya ya mmanja , komanso kuthyola nyumba ya Memory John ndi kubamo laptop yamtundu wa Lenovo zomwe ndi za ndalama zokwana 345 Thousand Kwacha.
Anthuwa anakadandaula kupolisi ndipo apolisi anayamba ntchito yafuna-funa nkuluyi ndikumugwira.
Popereka chigamulo chake First Grade Magistrate Roy Kakutu anati wapereka chigamulochi poofuna kuti ena atengerepo phunziro.
Issa Mussa amachokera mmudzi wa Sumaili mdera la mfumu yayikulu Jalasi mboma lomweli la Mangochi.
| 14 |
Amangidwa Kaamba Kogwililira Wamisala Wolemba: Thokozani Chapola rt-of-arrest.jpg 302w" sizes="(max-width: 586px) 100vw, 586px" /> Apolisi mboma la Chiradzulu amanga mkulu wina kaamba komuganizira kuti wagwililira msungwana wa zaka 17 yemwe ndi wamisala.
Wofalitsa nkhani za apolisi mbomalo Sergeant Yohane Tasowana watsimikiza za kumangidwa kwa mkuluyu Patrick Kodo polankhula ndi Radio Maria Malawi.
Iye wati zotsatira za kuchipatala zatsimikiza kuti msungwanayu anagwililidwadi ndipo Kodo akuyembekezeka kukawonekera ku bwalo la milandu posachedwapa.
Watsimikiza za nkhaniyi-Tasowana Woganiziridwayu anapita kunyumba kwa mtsikanayu madzulo ndipo anamugwiragwira ndi kumkokera patchire ndi kugona naye. Mayi ake a mtsikanayu ndi omwe anazanena za nkhaniyi ku polisi, anatero Sergeant Tasowana.
Iye wati milandu yogwililira ikuchulukira kwambiri mbomalo ponena kuti ikumakhala pafupifupi itatu pa mwezi uliwonse.
Kodo amachokera mmudzi mwa mpokera kwa mfumu yaikulu likoswe mboma lomwelo la chiradzulu.
| 7 |
Dayosizi ya Dedza Yakhazikisa Komiti Yolimbana ndi Mliri wa Coronavirus Dayosizi ya Dedza yakhazikitsa komiti yoyanganira ntchito zolimbana ndi mliri wa Coronavirus.
Poyankhula pambuyo pa msonkhano okhazikitsa komitiyi, mkulu woyendetsa ntchito za dayosiziyi bambo John Chithonje ati cholinga chokhazikitsa komiti ndi kugawana nzeru za momwe diayosiziyi ingalimbanirane ndi muliri-wu.
Ali nawo mu komitiyo-bambo Chithonje Mu komitiyi muli anthu ochokera mmagawo osiyanasiyana monga zaumoyo, zamaphunziro, za utumiki mu mpingo, atolankhani ndi ena. Bambo Chithonje akufotokoza.
Tayika task force imeneyi kuti igwire ntchito limodzi ndi boma, komanso ipindurira akhristu ngakhalenso atsogoleri a mpingo, anatero bambo Chithonje.
Ndipo mmawu ake wapampando wa komitiyi a Robin Ngalande omwenso ndi mkulu oyanganira ntchito za umoyo mu dayosizi ya Dedza ati athu onse amu dayosiziyo akuyenera kusatira njira zonse zomwe zikuperekedwa zopewera matendawa.
Tiwona ngati dayosizi yathu ngati mpingo ikutengapo mbali polimbana ndi matenda amenewa, sitisiyira boma lokha kulimbana ndi matenda amenewa ndipo mmalo mwake tigwira nawo ntchito limodzi, anatero a Ngalande.
| 6 |
CWO Ikulingalira Njira Zoyendetsera Bungweli mu Nyengo ya COVID-19 Bungwe la amayi mu mpingo wa katolika la Catholic Women Organisation (CWO) lati likulingalira za njira zatsopano zomwe zingathandize poyendetsera bungweli mu nyengo ino pomwe kwagwa mliri wa COVID-19.
Wapampando wa bungweli mayi Prudence Kadiwa ati akuluakulu a bungweli akumana posachedwapa kuti akambirane za mmene angayendetsere bungwe-li mu nyengo ino ya mlili wa COVID 19.
Ngati arkidayosizi ya Lilongwe tikhala ndi msonkhano wathu loweruka likubwerali pa 23 May kuti tikumane ndi kukambirana zoyenera kuchita maka pa zomwe tinalephera kupanga mu nthawi yake, anatero mayi Kadiwa.
Mayi Kadiwa anawonjezeranso ponena kuti mliri wa Coronavirus wasokoneza mapulani ochuluka a ntchito za bungwe-li.
Mliri umenewu usatibwezeretse mmbuyo pa moyo wathu wa chikhristu ifeyo ngati amayi. Chikhulupiliro chathu chikuyenera chikule ndinthu ngakhale tili pa mavuto amenewa, anatero mayi Kadiwa.
| 13 |
Ntchito za wedewede zanyanya Kusowa ndalama zoyendera zitukuko komanso kulekera anthu a kumudzi kugwira ntchito zomangamanga zachitukuko kukuchititsa kuti ntchitozi zizikhala zawedewede, atero akadaulo ena.
Izi zikudza patangotha sabata imodzi chipinda cha sukulu ya pulaimale ya Natchengwa ku Zomba chitagwa ndi kupha ophunzira 4 ndi kuvulaza ena. Mwezi watha, mlatho wina udadilizika galimoto ina ikudutsa ndipo anthu akhala akugawana zithunzi za msewu wosalongosoka mumzinda wa Lilongwe.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Zipinda za ku Nantchengwa zzidamangidwa ndi dothi Komiti ya zomangamanga ku Nyumba ya Malamulo ili ndi mphamvu zoyanganira ndi kuunikira pa momwe nyumba, misewu kapena milatho zikumangidwira kuti zizikhala zapamwamba ndi zolimba.
Koma wapampando wa komitiyo, Victor White Mbewe adati nthawi zambiri komitiyi imalephera kukwaniritsa ntchitoyi chifukwa imalandira thumba losakwanira kuzungulira dziko lonse kuyendera zitukuko.
Tikadakhala kuti timalandira thumba lokwanira, si bwenzi iyi ili nkhani chifukwa bwenzi tikumayenda paliponse kukaona momwe zitukuko zikuyendera. Zitukuko zambiri zikumangidwa ndi anthu akudera osayenderedwa, adatero Mbewe.
Mkulu wa bungwe la akatswiri a zomangamanga la Malawi Institute of Architects Mariam Mdooko wavomeleza kuti vuto lalikulu ndi loti nyumba zambiri zimamangidwa osafunsa ukadaulo wa ozidziwa.
Pali sukulu, zipatala, malo a bizinesi ndi nyumba zina zimene zikumangidwa osatsata ndondomeko. Ife akadaulo timadziwa zofunika ndi mamangidwe ake koma nthawi zambiri zimangomangidwa osatifunsa, adatero Mdooko.
Iye adati njira yokhayo yothanirana ndi vutoli nkuonetsetsa kuti ntchito yomanga isadayambike, akadaulo kaya a pakhonsolo kapena a mabungwe akuluakuluwa azifunsidwa.
Mneneri wa bungwe loyanganira ntchito zomangamanga mdziko muno la National Construction Industry Council Laison Gideon adati nthambiyo ili ndi malamulo omwe amayenera kutsatidwa kuchokera pachiyambi mpaka kumapeto.
Malamulo athu amati kontilakitala aliyense akuyenera kulembetsa mkaundula wathu. Ndipo ntchito iliyonse isadayambe tiuzidwe kuti tizitha kuyilondoloza ndipo timatero, adatero Gideon.
Iye adati ndondomeko izi sizitsatidwa nthawi zambiri chifukwa anthu ena amafuna kupanga zozemba koma sadziwa kuti zotsatira zake zimakhala zovuta ngati zomwe zimawonekazi.
Gulupu Matabwa, kwa T/A Chitekwere ku Lilongwe adati aphungu ndi makhansala amaika dyera ndi ndale patsogolo, zomwe zimadzetsa zitukuko zawedewede, zomwe zimathera mngozi ngati ya ku Zomba. Iye adati nthawi zina adindowa amadza ndi kontilakita wawowawo, mosemphana ndi amene komiti yachitukuko idasankha.
Komiti imatha kugwirizana wodzagwira ntchito ya chitukuko koma nthawi ikakwana, timangoona akubweretsapo munthu wawo. Timangozindikira katundu wafika ndipo ayamba kugwira ntchito, idatero mfumuyo.
Mkulu a bungwe loona kuti maphunziro ndi apamwamba, la Civil Society Coalition for Education (CSCE) Benedicto Kondowe wati kafukufuku wawo adapeza madera ambiri omwe anthu amadandaula kuti aphungu awo amawabweretsera kontilakitala komanso kuwagulira zipangizo osawafunsa maganizo awo.
Mlembi wamkulu muunduna wa za maboma angonoangono ndi chitukuko cha mmidzi Kiswell Dakamau adati mundondomeko ya mphamvu ku anthu, boma lidakhazikitsa ndondomeko ya momwe akadaulo aboma aziyanganira momwe zitukuko zikuyendera ndipo izi zikutheka.
Iye adati akati mphamvu ku anthu amangofuna kuti eni dera azitengapo mbali posankha chitukuko, kupeza malo komanso kuchita kalondolondo wa momwe ndalama zachitukuko cha mdera lawo zikugwirira ntchito.
Zinthu zikuyenda mmadera ambiri ndipo kunena kuti boma limalekerera anthu a kumudzi sizoona chifukwa chitukuko chilichonse chomwe chalowa mmabuku athu, chimakhala ndi wochiyanganira pokhapokha ngati sitikuchidziwa, adatero Dakamau.
Mkulu wa bungwe loyanganira za misewu Emmanuel Matabwa adati potsitira mgwirizano wa maiko a Sadc, nthambiyi idasintha kasankhidwe ka makontirakitala ndi kuunika ntchito.
Panopa kulibe zawedewede chifukwa tidamanga mabauti kuyambira pakasankhidwe ka makontilakitala, kuwapatsa mlingo omwe tikufuna ndi kuunika kuti akutsatiradi zomwe tawauzazo, adatero Matabwa.
Iye adati chitsanzo cha misewu yotere ndi wa Mzuzu-Nkhatabay omwe uli ndi milatho yolimba komanso ndi wotakasuka ndi wopsinjidwa bwino kuti usadzaonongeke msanga.
| 2 |
Za anamapopa sizikuzilala Nkhani ya anamapopa ikulephera kutha. Mtsogoleri wa dziko lino Peter Mutharika atangomaliza kuyendera maboma amene anthu angapo aphedwa powaganizira kuti ndi wopopa magazi.
Sabata yomweyi, munthu wina wa zaka 22 adaphedwa ku Chileka mumzinda wa Blantyre pomuganizira kuti ndiwopopa magazi. Anthu okwiya adaswa polisi ya pa Chatha kuderalo atamupeza atagona mmunda wina, chonsecho mkuluyo anali wakhunyu ndipo amachokera kuchipatala.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Mbale wa mfumu Mtenje, Henry Kawisa (Kumanja) kuyendera khola Ndipo mkulu winanso adaphedwa ku Balaka atapezeka akuyendayenda mbandakucha. Ndipo kwa Mtenje ku Chigumula mumzinda wa Blantyre, anthu adathyola khola la mfumu ya deralo ndi kubamo nkhumba 12, kuswa mawindo a nyumba yake mpaka kupulumutsidwa ndi apolisi.
Ndipo ena adachita zionetsero ngakhale pakati pausiku ku Bangwe, kwa Kachere, Machinjiri ndi Sigelege.
Zonsezitu zimachitika pomwe kuyambira Lachisanu mpaka Lolemba Mutharika adayendera maboma a Mulanje, Nsanje, Phalombe ndi Chiradzulu kumva anthu opulumuka ku opopa magazi, amene amaganiziridwa kuti ndi anamapopa komanso mafumu.
Chachikulu chimene chidatuluka pamisonkhanoyo nchoti mfumu yaikulu ya Alhomwe Paramount Ngolongoliwa idati akuchita izi ndi amatsenga ochokera ku Mozambique. Mfumuyo idapempha Mutharika kuti awasiyire zonse athane nawo mmatsenga.
Mundipatse masiku 21, ife mafumu anu tithana nawo. Sangamachoke ku Mozambique kudzatiseweretsa kuno ngati tilibe ufiti. Tithana nawo basi, adatero Ngolongoliwa.
Pamene adapempha Amalawi kusunga bata, makamaka pomwe akuganizira ena kukhala opopa magazi, Mutharika adati ngati nkhanizi ndi za matsenga azisiya mmanja mwa Ngolongoliwa ndi mafumu ena.
Koma mlembi wamkulu wa bungwe la oimira ena pamilandu la Malawi Law Society (MLS) Michael Goba wati ngati Ngolongoliwa adanena izi adaphwanya gawo 6 la malamulo okhudza nkhani za ufiti ndipo akhonza kumangidwa ndi kufunsidwa mafunso pakhoti.
Gawoli limati onena kapena zochita zake zikusonyeka kuti ndi mthakati kapena wochita zaufiti adzalipa $50 (K36 500) ndi kukhala kundende zaka 10. Zomwe akuti zidanenedwa ndi mfumuyo ndi mlandu. Malamulo ndi wothekera kuthana ndi vutoli pokhapokha adindo a mphamvu zotero atawagwiritsa bwino ntchito, adatero Chipeta.
Iye adati nzokhumudwitsa ngati Ngolongoliwa adanenadi izi chifukwa udindo wake ndi wolemekezeka komanso uli pansi pa malamulo a dziko lino.
Pankhani yokhudza ufiti mdziko muno, Chipeta adati polingalira mwakuya ndi povuta kunena kuti ulipo kapena ayo chifukwa ngati chipembedzo zimatengera katanthauziridwe ka mphamvu zapaderazi ndi zikhulupiriro za anthu. Iye adaonjezeranso kuti pachifukwachi sunganeneretu kuti munthu angachite kapena kusachita ufiti mdziko lomwe silivomereza mchitidwewu.
Malingana ndi mkulu wa bungwe la Association of Secular Humanism (ASH) George Thindwa, yemwe amalimbikitsa ganizo loti ufiti kulibe, Ngolongoliwa sadathandize kuthana ndi mpheketserayi ndipo amayenera kutsata malamulo a dziko lino chifukwa anamapopawo kulibe.
| 19 |
Wapitadi Gwanda Ngati bodza Lachisanu lapitali walowadi mmanda Gwanda Chakuamba, mmodzi mwa amkhalakale pandale mdziko muno.
Mmene chitanda cha malemu Chakuambayemwe mmaboma a Nsanje ndi Chikwawa kuchigwa cha Shire ankamutcha Mbuya pomulemekeza chifukwa cha zabwino zambiri zomwe adakhala akuchitira anthu a kuchigwachi ali moyo, chimatsikira mmanda ku Chinyanje kwa T/A Mlolo, kuseri kwa nyumba yake yotchedwa Zuwele Castleambiri sadathe kuigwira misozi.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Maliro a Chakuamba adalandira ulemu wapadera poikidwa ndi asirikali a nkhondo a MDF Ndi mitima yosweka ambiri adalira: Wapita Mbuya, wapita Mbuya! Amayi a Dorica a Muona Seventh Day Adventist adaimba mobwerezabwereza: A Chakuamba ku Nsanje, a Chakuamba ku Chikwawa kutanthauza kuti Chakuamba adali mwana wa maboma awiriwa.
Mizwanya ina yodziwika pandale yomwe idabwera kudzaperekeza Mwana Mphenzi ndi mtsogoleri wakale Bakili Muluzi, Sipika wakale Chimunthu Banda, Brown Mpinganjira, Sidik Mia, Kamlepo Kalua, Nicholas Dausi, Harry Thomson, Bazuka Mhango, akuluakulu a zipani za MCP, UDF ndi DPP ndi akuluakulu a boma motsogozedwa ndi mlembi wamkulu mu ofesi ya Pulezidenti ndi Kabineti George Mkondiwa, kungotchurapo ena pangono.
Inde kudali chinamtindi cha anthuolira ndi ongoyangana, amipingo yosiyanasiyana ndi osapemphera omwe, koma onse okhala ndi cholinga chimodzi: kudzaperekeza munthu yemwe mbiri yake sidzaiwalika mmbiri ya dziko la Malawi ngati mmodzi mwa anthu amene adamenyera ufulu wa dziko lino kuchoka mmanja mwa atsamunda kufikira lero lino pamene dzikoli lili paufulu wodzilamulira.
T/A Malemia amene adalankhula mmalo mwa T/A Mlolo pamaliropo, adati ngakhale akulira, koma ndi osangalala kuti kudera la chigwa cha Shire kudachoka munthu wodzipereka ndi wokonda anthu ake ngati Chakuamba yemwe dziko la Malawi silidzamuiwala.
Sitidzapezanso Chakuamba wina kuno. Uyu ndiye adali weniweni; wangwiro, wachilungamo, wosaopa, mkhalakale pandale. Watiphunzitsa kukhululukirana ndi kugwirana manja ngati tifuna kuti dziko lathu litukuke. Uku kudali kulira kwa Paramount Lundu.
Ena adayerekeza Chakuamba ndi malemu Nelson Mandela mtsogoleri wakale wa dziko la South Africa, pokhululukira chipani cha MCP, chomwe chidamangitsa nkumuponya mndende kwa zaka 14, koma atatuluka kundendeko adalowanso chipani chomwecho nkumagwira ntchito limodzi ndi omwe adamum-angitsawo.
Pa ichi, Malemia adati Chakuamba adali munthu wosasunga mangawa ndipo ankalankhula akaona kuti zinthu zikulakwika, zomwe zinkamuika mmavuto nthawi zambiri.
Chakuamba adali wokonda sukulu ndipo kuno waphunzitsa anthu ambiri, Malemia adatero.
Ndipo ena mwa mafumu omwe Msangulutso udacheza nawo adati dziko lino lataya mkhalakale pandale yemwe adatengapo gawo lalikulu pothandizira kulitukula komanso yemwe adali wovuta kumumvetsa pakachitidwe kake mundale.
Inkosi Chindi ya mboma la Mzimba idati idadzidzimuka itamva za imfa ya Chakuamba pawailesi Lolemba lapitali kaamba koti simadziwa zoti wakhala akudwala kwa kanthawi.
Chindi adagwirizana ndi mafumu anzake kuti Chakuamba adali wachitukuko.
Adali munthu wabwino ngakhale munthawi ya ulamuliro wa MCP adali watinkhanza pangono. Paja adadzamenya mafumu kuno kumpoto pamsonkhano waukulu wa chipani mu 1973 ku Marymount mumzinda wa Mzuzu, adatero Chindi.
Iye adati mmodzi mwa mafumu omwe adapatsidwa makofi adali bambo ake chifukwa adakana kupereka ngombe ngati mphatso kwa Kamuzu.
Ndipo mfumu yaikulu Mkukula ya mboma la Lilongwe idati sidzamuiwala Chakuamba chifukwa cha momwe adagwirira ntchito panthawi yothetsa bungwe la MYP.
Mkukula adati Chakuamba ngati mmodzi mwa akuluakulu a boma, adalolera kukambirana ndi kulithetsa bungweli bwino lomwe popanda zipolowe zambiri.
Mmodzi mwa otsata za ndale mdziko muno, Humphrey Mvula, adati Chakuamba adamenyera ufulu wa dziko lino kuchokera nthawi ya atsamunda mpaka nthawi yomwe dziko lino lidathana ndi ulamuliro wa chipani chimodzi.
Malinga ndi Mvula, Chakuamba adali wolimba mtima ndipo sadali wosankha mitundu ngati momwe achitira andale ena omwe amakokera kwawo.
Mvula adati ngakhale Chakuamba sadapambaneko chisankho a mtsogoleri wa dziko lino, adatsala pangono kupambana mchaka cha 2004 pomwe adaimira Mgwirizano Coalition.
Chakuamba adatsikira kuli chete Lolemba lapitali pachipatala cha Blantyre Adventist (BAH) mu mzinda wa Blantyre, naikudwa mmanda ndi ulemu wa asirikali ankhondo.
| 11 |
Kuyamba kwa zipolowe Malipoti mdziko la South Africa akhala akumveka kuti mfumu ya mtundu wa Chizulu Gooodwill Zwelithini ndiyo idakolezera moto pamene idalankhula kuti mzika za mmaiko ena zibwerere kwawo ponena kuti zikuwaphangira ntchito. Malipotiwo adati pamsonkhano wina ku Polonga mdzikolo, mfumuyo idati anthu achilendo,a mene amatchedwa makwerekwere ku South Africa apakire tawo nkubwerera kumudzi.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Malipotiwa atangomveka, anthu obwera akhala akuona zakuda ndi mzika za mdzikomo ndipo anthu oposa 7 aphedwa, mwa iwo awiri ndi a mdziko muno ndi ena kuvulazidwa.
Ngakhale utsi sufuka popanda moto, Lolemba Zwelithini adakana izi pamene amalankhula pabwalo la Moses Mabhida ataitanitsa mafumu, mamulumuzana ndi ena onse mdzikomo ndipo adati atolankhani ndiwo sadamumvetse zomwe ankanena.
Maiko komanso mabungwe mu Africa akhala akudzudzula zomwe zikuchitika mdzikolo.
Dziko la Nigeria nalo lidayamba kusala nzika za dziko la South Africa moti pofika Lachitatu, ofesi ya kazembe wa South Africa ku Nigeria adaitseka.. Ku Zimbabwe, wailesi za mdzikolo zidasiya kuimba nyimbo za mdziko la South Africa. Pamene ku Mozambique, nzika zina za mdziko la South Africa zidachitidwa chipongwe ndipo galimoto zina za ku South Africa zidatenthedwa..
Ku Malawi anthu adachita zionetsero Lachiwiri pamene adakapereka chikalata cha madandaulo awo kwa kazembe wa dziko la South Africa.
| 11 |
Kwaipa ku chipatala, mankhwala atha Mwa mankhwala 100 amene amayenera kupezeka mzipatala za boma, asanu okha ndiwo alipo, Nduna ya Zaumoyo Catherine Gotani-Hara idatero ku Lilongwe Lolemba.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Polankhula akulandira mankhwala osiyanasiyana a ndalama zokwanira K170 miliyoni kuchokera ku bungwe la AmeriCares, Gotani-Hara adati kusowa mankhwala mzipatala za boma kwankitsa.
Mankhwala akusowa chonchi chifukwa chigulireni mankhwala ochuluka mu 2009, boma silinagulenso mankhwala. Awa adali mankhwala okwanira chaka chimodzi, idatero ndunayo.
Kusowa mankhwala kwafika pena mpaka madotolo 15 adalembera kalata mtsogoleri wa dziko lino Joyce Banda kuti achitepo kanthu pa zakusowa kwa mankhwala chifukwa ena akumwalira ndi nthenda zochizika.
Mkulu woyanganira nkhokwe za mankhwala Feston Kaupa adati mankhwala afikawo sachedwa kutha chifukwa aperekedwa kwa anthu amene samalandira mmbuyomu.
Mkulu wa mgwirizano wa mabungwe oona za umoyo la Malawi Health Equity Network (Mehn) Martha Kwataine naye adati zanyanya ndipo adati walembera komiti ya zaumoyo ndi younikira za bajeti ku Nyumba ya Malamulo kuti alingalire zakuti zipatala zikuluzikulu zizingopereka mankhwala a nthenda za mgonagona basi.
| 6 |
Joyce Mhango: Nyale ya zisudzo Azisudzo mMalawi muno akhala akulimbika kutukula lusoli koma chifukwa cha zovuta zina ndi zina mwayi woonekera nkulandira mphotho pa zochita zawo sumapezeka. Ena adayamba kutaya mtima kuti Malawi ingapange zisudzo zoti maiko ena nkutamanda. Izi zili choncho, masiku apitawa, mmodzi mwa ochita zisudzo mMalawi muno, Joyce Mhango, adalandira chikho cha ulemu pa ochita zisudzo a mmaiko osiyanasiyana a mu Africa. STEVEN PEMBAMOYO adacheza naye pa nkhani yabwinoyi.
Poyamba tafotokoza kuti ndiwe ndani? Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Kusonyeza chikho chake: Chavula-Mhango Ndine Joyce Mhango Chavula wochokera ku Rumphi. Ndidasankha kukhala wa zisudzo mmoyo mwanga. Makamaka ndimapanga mafilimu, kuchita zisudzo, kukhala mkonzi wa zisudzo komanso ndimayendetsa kampani ya zisudzo ya Rising Choreos.
Posachedwapa udalandira chikho kukuyamika pa ntchito yako makamaka chifukwa cha filimu yako yotchedwa Lilongwe. Amalawi ambiri ndiwonyadira chifukwa cha nkhaniyo koma sadziwa kuti filimuyi ndiyotani. Ungawafotokozere? Zoonadi ambiri mwina sakuidziwa bwino filimuyi. Lilongwe ndi filimu yomwe imakamba za mtsikana oyendayenda yemwe ali ndi ana atatu omwe adapatsidwa ndi amuna osiyanasiyana. Iye ali pantchito yabwino koma amapeza ndalama zambiri kuchoka kwa amuna okwatira omwe amagona nawo. Pambuyo pa zaka 7 kale lake la Lilongwe lidayamba kumuweruza ndipo mufilimu yonse samaiwala mawu oti Musandiweruze chifukwa simukudziwa komwe ndachokera.
Bwanji sitidamveko kuti wakhazikitsa filimi imeneyi mdziko muno? Idakhazikitsidwa mu October chaka chatha ku Lilongwe ku Cinema koma anthu ambiri adasemphana nayo. Mapulani okhazikitsanso alipo mu April chaka chino kuti anthu adzayionerere ndipo chimbale chake chifika pamsika posachedwapa.
Udalandira ulemu waukulutu koma ukuona ngati chinsinsi chake chagona pati? Ndiyambe ndi kunena kuti ndine wodala kukhala mmodzi mwa olandira ulemu umenewu. Ndidapereka filimuyi kwa woyendetsa mwambo kuti ipikisane nawo ndi mafilimu ena ndipo mwa mwayi idasankhidwa kukhala nawo mgulu la mafilimu omwe adasankhidwa. Ndimakhulupilira kuti kulimba mtima kwanga ndiko kudandithandiza pamphepete pa madalitso a Mulungu.
Zidakutengera nthawi yaitali bwanji kupanga filimuyi ndipo udakumana ndi zokhoma zanji? Zidatitengera masiku 12 ojambula mosadukiza koma kuti zonse zitheke padatenga nthawi yaitali. Nthawi yovuta kwambiri idali yokonzekera; kusankha anthu oyenera, kusonkhanitsa zofunika ndingoti padalibe kugona. Komabe zonsezo zidapita poti filimuyi yalandirako zikho ziwiri tsopano. Choyamba cha ochita zisudzo mwapamwamba ku Shunaffoz ku Zambia mchaka cha 2015 ndi ichi chapompanochi.
| 9 |
Apalamula poitana T/A kumwambo pafoni Mwambo wobzala mitengo ku Bula mboma la Nkhata Bay udasokonekera Lachinayi pamene mfumu yaikulu Mbwana idakana kupita kumwambowu ati kaamba koti okonza mwambowo sadatsate dongosolo loitanira mfumu.
Mwambowu, womwe adakonza ndi a nthambi ya zankhalango mogwirizana ndi bungwe la Temwa, udaima ndi pafupifupi mphindi 30.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Apatu nkuti akuluakuluwo akukambirana za tsogolo la mwambowo ndi wapampando wa chitukuko kumeneko, Ivol Nyirenda, yemwe adabweretsa uthengawo.
Mlendo wolemekezeka pamwambowo, yemwe ndi wapampando wa khonsolo ya Nkhata Bay, Hastings Mkandawire, pamodzi ndi akuluakulu ena a boma, adangoti kakasi kusowa chochita poti zawo zinali zitada.
Nawo ana asukulu pamodzi ndi anthu ena onse oitanidwa adali nyominyomi pamalopo, pomwe ena adangokhala pansi kudikira za zotsatira za zokambiranazo.
Uwutu udali mwambo waukulu wokhazikitsa nyengo yobzala mitengo mchigawo cha kumpoto.
Koma nkhope za anthuwo zidawala patatha mphindi 30 pomwe adaona T/A Mbwana ikutulukira mgalimoto ya mtundu woyera. Mukucheza kwathu ndi Mbwana, mfumuyi idakana kukambapo zambiri pankhaniyo ati pokana kuwaika mmavuto omwe adakonza mwambowo.
Afunseni omwe akonza mwambo uno, ndikayankha ine, ndingawaike mmavuto, idatero mfumuyo.
Koma Mkandawire, yemwe adabweretsa uthengawo, adati anthuwo sadatsate dongosolo poitana mfumuyo kumwambowo.
Simungaitane mfumu kumwambo ngati uno kudzera palamya, iye adatero.
Ndipo polankhulapo, mmodzi mwa okonza mwambowo, woimira DC wa boma la Nkhata Bay, Mzondi Moyo, adati zoti dongosolo silidatsatidwe sizidali zoona.
A kunthambi ya zankhalango adatsata dongosolo poitana mfumuyi komanso tidapereka udindo woitana mfumuyi kwa a bungwe la Temwa omwe amakhala nayo pafupi kwambiri, adatero Moyo.
Mitengo yokwana pafupifupi 8 miliyoni ibzalidwa chaka chino mnyengo yobzala mitengo mchigawochi.
| 8 |
Akhristu Ali ndi Udindo Wosamalira Chilengedwe-Bambo Chilolo Vicar general wa dayosizi ya Zomba, bambo Vincent Chilolo ati akhristu ali ndi udindo waukulu wosamalira chilengedwe chomwe ndi chofunika kwambiri pa moyo wa munthu.
Bambo Chilolo amayankhula izi loweruka ku St. Charles Lwanga Parish pomwe akhristu a parishi-yi amakhadzikitsa ntchito yodzala mitengo.
Iwo ati parishi-yo Iwonetsetsa kuti mitengo yomwe yadzalidwayi ikusamalidwa bwino kuti cholinga chodzalira mitengoyi chikwanilitsidwe.
Chaka ndi chaka timadzala mitengo koma pena timatayilira kusayisamalira. Ndiye tikufuna kuti mitengo imeneyi isamalidwe bwino kuti ikule ndi kukwaniritsa cholinga chathu, anatero bamboo Chilolo.
Mau ake Moderator wa St. Charles Lwanga Parish, mayi Immaculate Chamangwana anati achita izi pofuna kukwanilitsa imodzi mwa mfundo za masomphenya a dayosizi yawo ya Zomba.
| 18 |
Abzala mitengo ku Neno Kukuphopholedwa mitengo ku Neno. Makala ambiri akuti akuchokera mbomalo, malinga ndi mkulu woyanganira nkhalango kumeneko.
Chifukwa cha ichi, mkuluyo, Emmanuel Ngwangwa, komanso DC wa bomalo, Memory Kaleso Monteiro, Lachitatu adatsogolera kubzala mitengo mmudzi mwa Hiwa kwa T/A Chekucheku.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Patsikulo, mitengo 1 200 ndiyo idabzalidwa ndipo chiyembekezo nchakuti pakutha pa chaka chino abzale mitengo 750 000 kusiyana ndi chaka chatha pamene adabzala mitengo pafupifupi 500 000.
Ngwangwa adati ngakhale chaka ndi chaka akubzala mitengo, imene ikupulumuka ndi yochepa chifukwa cha anthu amene amatentha nkhalango komanso amene amadyetsera ziweto paliponse.
Tauza mafumu kuti aonetsetse kuti zotere zachepa. Komanso tauza aliyense kuti abzale mtengo umodzi pa chaka. Atha kuposera apa koma tikufuna kuti aliyense atengepo mbali pobzala mitengo, adatero Ngwangwa.
Bungwe la Shire River Basin Management Project ndilo lidapereka thandizo la mitengoyi komanso thandizo loti pakhale kukumana pakati pa akuluakuluwa ndi anthu awo.
| 18 |
Anthu Atenge Gawo Pothana ndi Kusintha kwa Nyengo-CADECOM Bungwe loona za chitukuko mu mpingo wakatolika la CADECOM lati anthu akumudzi akuyenera kutenga gawo lalikulu pofuna kuthana ndi mavuto omwe amadza kaamba kakusintha kwa nyengo mdziko muno.
Kusintha kwa nyengo kukubweretsa mavuto ngati awa Mmodzi mwa akuluakulu ku bungwe-li kuchokera ku likulu la mpingo wakatolika mdziko muno a Aron Kandiwo Ntaya, ndi omwe izi lachinai pa mkumano omwe bungweli linali nawo ndi anthu a mdera la Senior Chief Liwonde mboma la Machinga, pomwe amafuna kudziwa ena mwa mavuto omwe anthuwa akukuma nawo kaamba ka kusintha kwa kanyengo.
Iwo ati apitiliza kuthandiza anthu mderali ndi cholinga chofuna kuchepetsa mavuto omwe akukumana nawo kaamba kakuonongeka kwa chilengedwe ndi kuwapatsa maphunziro a mmene angabwezeretsere chilengedwe komanso.
Tikufuna tiwapatse mphamvu kuti akwanitse kupeza kangachepe pakhomo pawo ndi kuthana ndi kusintha kwa nyengo, anatero a Kandiwo.
Polankhulapo a Dalisto Tengani omwe ndi mmodzi mwa anthu amene ali amayanganira nkhani zakusintha kwa nyengo ati anthu mderali akukumana ndi mavuto ambiri omwenso mwazina akupangitsa kuti aphwanyilidwe maufulu awo.
Abambo tikukumana ndi mavuto. Tikukanika kuchita zofuna zathu pamoyo wathu chifukwa njalayi ikuchititsa kuti tizipita ku Mozambique kukasaka maganyu komwenso timavutika kwambiri, anatero a Tengani.
| 18 |
Dayosizi ya Chikwawa Ili ndi Komiti Yatsopano ya Abwenzi a Radio Maria By Richard Makombe Abwenzi a Radio Maria Malawi mu dayosizi ya Chikwawa asankha komiti yatsopano yomwe cholinga chake ndikuthandiza kuyendetsa ntchito za Radio Maria.
Komitiyi yasankhidwa pambuyo pa chisankho chomwe abwenzi a wayilesiyi anakonza chomwe chinachitikira loweruka ku St. Michaels Cathedral mboma la Chikwawa.
Poyankhula pa mbuyo pa masankhowa, a National Coordinator a Radio Maria a Louis Phiri ayamikira abwenzi a wayilesiyi mu dayosiziyi kamba kotuluka mwaunyinji ndi kusankha atsogoleri a ku mtima kwawo.
A Phiri alimbikitsa abwenzi onse amene asankhidwa kukhala mu komiti yatsopano ya dayosizi ya Chikwawa kuti asabwelere mbuyo pogwira ntchito yawo.
Ndithokoze kwambiri nonse amene munatenga nawo mbali powonesetsa kuti chisankhochi chiyende bwino komanso mwa bata ndi mtendereanatero a Phiri.
A Phiri anatengerapo mwayi ndikupempha atsogoleri atsopanowa kuti akonzekere bwino ndikuadzatenga nawo mbali pa chikondwelero chokumbukira kuti Radio Maria Malawi yakwanitsa zaka 20 ikufalitsa uthenga wabwino mdziko muno chomwe chidzachitike mwezi wa September chaka chino..
Pothilirapo ndemanga wapa mpando wa Laity Council mu dayosizi ya Chikwawa a George Mkutu anayamikira abwenzi a Radio Maria mdziko muno kamba kotenga gawo pa ntchito zothandiza Radio Maria mdziko muno.
Ndikofunika kuti abwenzi a Radio Maria akhale patsogolo kuthandiza wayilesiyi kaamba koti thandizo kwa akhristu ndi anthu onse mdziko muno choncho ngati abwenzi a wayilesiyi akuyenera kutsogolera pa ntchito yothandiza wayilesiyi, anatero a Mkutu.
Mmawu ake wachiwiri kwa wapampando yemwe wasankhidwa kumene a Clement Majawa ati ndiokondwa kuti komiti yomwe amayiyembekezera tsopano yasankhidwa.
Ena omwe asankhidwa mmaudindo ndi monga a Mathews Chimota omwe ndi wapampando, Clement Mjawa asankhidwa kukhala wachiwiri kwa wapampando, ndipo a Zachariah Malunga awasankha kukhala mlembi ndipo wachiwiri wawo ndi a Cecelia Jeke komanso a Enifa Mwale awasankha kukhala msungichuma.
| 13 |
Auka atatha zaka 11 mmanda ku ntchisi Pa 16 April 2005 lidali tsiku lachisoni mmudzi mwa Ngwanje, T/A Malenga mboma la Ntchisi pomwe mayi Nkomanyama Charles adamwalira akubereka mwana wake wa nambala 6.
Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Zaka 11 chichitikireni izi, zodabwitsa zaoneka mmudzimo pomwe munthu amene akumuganizira kuti ndi malemuyo adapezeka ali zungulizunguli mmphepete mwa phiri la Katsumbi mawa wa pa 13 February ali moyo.
Mneneri wa apolisi mbomalo Gladson Mbumpha, watsimikiza za nkhaniyi ndipo wati pano mayiyo ali kwa amene akuti ndi makolo ake.
Anthu akukhamukira ku Ntchisi kukaona Nkomanyama Malinga ndi Mbumpha, apolisi adali amkhalapakati wa zokambirana pakati pa mafumu ndi makolo a mayiyo kuti amulandire.
Poyamba mayi ake omwe ndi a mmudzi mwa Chithonje ankachita naye mantha moti ankasungidwa ndi mfumu Katipwiri kufikira titamaliza zokambirana pa 15 February, adatero Mbumpha.
Mayiyo atangopezeka, yemwe akuti ndi mwamuna wake, Yobu Gwaza, wa mmudzi mwa Ngwanje, ndiye adayamba kumuzindikira ndipo adafotokoza kuti mkazi wakeyo adamwalira mchaka cha 2005 akubereka Dorica, mwana wawo womaliza yemwe ali moyobe mpaka pano.
Iye adati adalera yekha mwanayo ndipo chithunzithunzi cha mkazi wakeyo chidali chikadali mmutu nchifukwa chake sadachedwe kumuzindikira atamuona.
Gwaza adati alibe vuto lililonse ndi mkazi wakeyo ndipo ndi wokonzeka kumulandira akapeza thandizo nkubwerera munzeru zake bwinobwino.
Ngati angachire nkukhala bwinobwino chomuletsera kubwerera pakhomo pake nchiyani? Mmesa ana ake ali kunyumba komweko? adatero Gwaza.
Anthu akukhamukira kukaona zozizwitsazo, ye,we akuti ndi malume a mayiyo, Masaiti Kalulu, atabweretsa chithunzi chomwe Nkomanyama adajambulitsa asadafe ndipo anthu omwe adachiona kuphatikizapo apolisi akuti pali kufanana pakati pa nkhope ya pachithunziyo ndi mayiyo.
Mbumpha adati anthuwo ataona chithunzicho adakwiya ndi kukana kwa mayi a woukayo ndipo pamalopo padayamba phokoso lomwe adakaletsa ndi apolisi.
Padali chisokonezo moti chipanda apolisi kufika msanga, pakadachitika chachikulu mwinanso mpaka mayiyo akadamenyedwa, adatero. Padakalipano mayi akumuganizira kuti adaukayo ali kwa mayi ake koma akuti sakutha kuyankhula komanso nthawi zina amadya mwachidodo.
Tikukhala naye bwinobwino ngakhale kuti pena amachita zinthu mwachidodo monga kudya. Akhoza kuyamba pano koma kuti amalize pakumatenga nthawi.
Vuto lina lomwe lilipo ndi losatha kuyankhula ndiye nzovuta kudziwa chomwe akufuna. Tiona kuti akhala bwanji tikayenda naye, adatero mayi Charles.
Mfumu Chithonje ya mmudzi momwe mumachokeratu makolo a mayiyo idatsimikiza za maliro a mayiyo ponena kuti ngoziyo itachita mchaka cha 2005, idalandira uthenga ndipo idachita nawo mwambo wa malirowo.
Mfumuyo idati kawirikawiri nkhani zokhudza munthu womwalira nkupezeka ali moyo zimazunguza mutu ndiponso zimayambitsa phokoso anthu akazitengera pamgongo.
Pakalipano apolisi alangiza mafumu ozungulira derali kuti aphe tsiku kupita kukanda kuti akatsimikize ngatidi mmanda momwe adaika mtembo wa Nkomanyama Charles mulibedi thpi lake.
Mkulu wina wa mpingo wa Church of Christ mboma la Nkhotakota, Maxwel Nangunde, adati amakhulupirira kuti munthu akamwalira basi kwake kwatha mpaka patsiku la chiweruzo.
Zina ukamva abale koma mpovuta kunena kuti chenicheni nchiti chifukwa anthufe timakhulupirira kuti munthu akapita wapita basi mpaka tsiku la chiweruzo, adatero Nangunde.
Koma mmbiri ya chilengedwe tikumva za kuuka kwa akufa kwa Yesu Khristu amenenso adaukitsapo anthu angapo monga Lazalo, mwana wa Jairus kudzanso mnyamata wina wa mayi wamasiye ku Nain.
Tikumvanso kuti pamene Yesu adapachikidwa pamtanda, adaukanso patapita masiku anayi ndipo adalowa mlimbo naukitsa matupi a anthu abwino omwe adafa.
Komanso mbuku la chipangano chakale tikuwerenga za mmene mneneri Eliya adaukitsira mwana wa namfedwa wa Zarephath; Elisha naye adaukitsa mwana wa mkazi wina Mshunammite kwa akufa.
Naye Paulo akuti adaukitsikwa kwa akufa atagedendwa ndi miyala ndi anthu a ku Antioch ndi Iconium nkumusiya ali thapsa! Komanso Paulo yemwenso akuti adaukitsa Eutychus yemwe adafa atagwa pansi kuchokera panyumba yosanjikizana mmene ankatsinza.
Petulo nayenso adaukitsa mayi wa ntchito zabwino dzina lake Tabitha wa ku Joppa, yemwe amatchedwanso kuti Dorcas, atamwalira nkuikidwa mmanda.
| 19 |
Cashgate isokoneza khisimisi kwa a mboma Ogwira ntchito mboma kutchinga maofesi awo ku Lilongwe Anthu ambiri ogwira ntchito mboma ali pachiwopsezo chakuti Khisimisi ya chaka chino saiwona bwino chifukwa chosowa ndalama anthu ena ogwira ntchito mboma ataba ndalama zankhaninkhani.
Mpaka pano nthambi zina za boma, monga kuunduna wa zamaphunziro, sadalandirebe ndalama za November ndipo pali chikayiko kuti pofika tsiku la Khisimisi mmasiku anayi akudzawa akhala atalandira ndalama zawo.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Bungwe loyanganira ufulu wa anthu ogwira ntchito mboma la Civil Service Trade Union (CSTU) lati ogwira ntchito mboma omwe sadalandire ndalamawo akuzunzika chifukwa anthu ena adaba ndalama za boma, nkhani yomwe pano ikudziwika kuti Cashgate.
Mtsogoleli wa bungweli, Eliah Kamphinda-Banda, wati nzomvetsa chisoni kuti anthu akuzunzika pomwe ndalama zawo zili mmatumba a anthu ena ndipo wati boma liganize mozama pankhaniyi ndi kuthandiza anthuwa mwamsanga.
Sizimayenera kukhala choncho koma vuto ndi lakuti anthu ena amaganizo olakwika adaba ndalama za boma, nchifukwa chake anthu ena ogwira ntchito mboma akuvutika chonchi, adatero kamphinda-Banda pouza Tamvani.
Boniface Mbowe ndi mmodzi mwa aphunzitsi pasukulu ya Kabyala ku Mchinji yemwe akuti mpakana pano sadalandirebe malipiro ake ndipo wati izi zamulowetsa mungongole zankhaninkhani.
Ndidachita kubwereka ndalama zolipira nyumba ndi ndalama zoti ana ayendere kuchoka kusukulu. Pakalipano ndikusowa ndi ndalama yogula mbewu moti mwina ndibzala mbewu yakabwereza. Mukanena za Khisimisi ndiye iwalani chifukwa olo ndalama zitabwera lero zonse zipita kungongole, adatero Mbowe.
Nduna yoona kuti ulamuliro ukuyenda bwino mu Ofesi ya Pulezidenti ndi Nduna, Chris Daza, wati malipirowa achedwa chifukwa boma limakonza makina atsopano owerengera ndalama za boma.
Iye wati anthu omwe sadalandirebe ndalama zawo asade nkhawa chifukwa ntchito yokonza makinawo ili kumapeto koma sadanene tsiku lomwe anthu angakhale atalandira malipiro awo.
Vuto la kuchedwa ndi kuchepa kwa malipiro labweretsa mavuto osiyanasiyana mdziko muno kuphatikizapo kumwalira kwa anthu mzipatala chifukwa cha masitalaka omwe ogwira ntchito za umoyo akhala akupanga.
Mabungwe omwe si aboma komanso maiko omwe amathandiza dziko lino akhala akudzudzula boma kaamba kolephela kulimbikitsa ogwira ntchito mboma makamaka pankhani ya malipiro.
Mtsogoleri wa bungwe loona za ufulu wa anthu ogula malonda la Consumers Association of Malawi (Cama) John Kapito wati ndi mmene katundu akukwerera mtengo masiku ano moyo wa munthu ngofunika ndalama zokwanira kuti amasuke.
Panopa ngakhale chithandizo cha kuchipatala chikukomera omwe ali ndi ndalama tsono mukaikapo lendi, zovala ndi chakudya munthu akufunika ndalama zingati? Ngati pavuta ndi bwino kuti munthu amupatseko zofunikira kwambirizo koma osati kungomutayiratu, adatero Kapito.
Mneneri wa nthambi yowongolera chuma cha boma, Nations Msowoya, wati vuto la kuchedwa kwa malipiro lidaonekeratu kuyambira pomwe kufooka kwa ndondomeko yoyendetsera chuma cha boma ya Integrated Financial Management Information System (Ifmis) kudaonekera poyera.
Mavuto awa adawonekeratu titangotulukira kufooka kwa ndondomeko yomwe boma limatsata poyendetsa chuma ya Ifmis, choncho sitikudabwa, koma zonse zilongosoka, adatero Msowoya.
Iye akuti pofika Lolemba lathali aphunzitsi ndi ogwira ntchito kuunduna wofalitsa nkhani ochokera ku Ntchisi, Mulanje, Mangochi ndi Phalombe adali asadalandire malipiro a mwezi wa November.
Msowoya adati ngakhale kuti mlembi wamkulu wa boma Hawa Ndilowe adalemba kalata yoti ogwira ntchito mboma alandire malipiro pofika pa 16 December, ambiri sadalandirebe koma adati boma liyesetsa kuti alandire malipiro a December pofika masiku a chisangalalo cha Khisimisi.
Koma mlembi wa mkulu wa bungwe la aphunzitsi la Teachers Union of Malawi (TUM) Denis Kalekeni wati nzokhumudwitsa kuti aphunzitsi nthawi zonse amaikidwa kumapeto pankhani yolandira malipiro.
Iye wati aphunzitsi 1 065 ochokera ku South East Education Division, 1 083 ochokera kunthambi ya maphunziro ya boma la Ntchisi kuphatikizapo aphunzitsi a ku Kochirira CDSS, Minga CDSS ndi ena ochokera kunthambi ya maphunziro ya boma la Mulanje sadalandirebe malipiro awo a mwezi wa November.
Kalekeni wati bungwe la aphunzitsi lidalemba chikalata kuunduna wa zamaphunziro kuti aphunzitsi omwe azikhala asadalandire ndalama zawo pakadutsa pa 27 azinyanyala ntchito koma unduna sudayankhe chibaluwacho.
Kalatayo idapita koma sadatiyankhe moti pano chomwe chatsala ndi kuti tiyambe kuwadziwitsa aphunzitsi za nkhaniyi chifukwa ambiri sakudziwapo kanthu, adatero Kalekeni.
| 10 |
Ndende zisanduka makhoti Zanathina mmabwalo a milandu. Sitalaka ya ogwira ntchito mmabwalowa idasandutsa zitokosi za polisi kukhala mabwalo ozengera milandu.
Izi zimachitika akuluakulu a mabwalowa atalephera kunyengerera ogwira ntchito kuti asiye sitalakayi ndi kubwerera kuntchito.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Mkulu wa makhoti Andrew Nyirenda adapempha oweruza milandu onse kuti ayambe kuweruzira milandu kupolisi ndi kundende.
Nyirenda adapempha mamajisitiliti kuti agawane ntchito kuti ena azimasulira chigamulo, ena azilemba ndipo ena azinyamula mafailo, ntchito zomwe zimagwiridwa ndi owathandizira.
Ofesi ya mkulu wa makhoti ikudziwitsa kuti malinga ndi sitalaka yomwe ikuchitikayi, mukupemphedwa kuti muyambe kumva milandu ndipo ngati nkotheka muzipereka belo, udatero uthenga wa Nyirenda.
Kutsatira uthengawu, mamajisitileti adayamba kuzenga milandu, komanso kupereka belo kwa anthu oganiziridwa kuti adapalamula milandu omwe amasungidwa mzitolokosi.
Kupolisi ya ku Limbe mu mzinda wa Blantyre, mamajesitilitiwa adatulutsa anthu angapo pa belo, komanso kumva milandu yosinasiyana. Izi zimachitikira mchitolokosi.
Nako ku Dedza, mamajesitilitiwa adapatsidwa ofesi yapadera momwe amagwiritsiramo ntchito ngati khoti.
Majesitiliti wina akamaweruza mlandu, mnzake amatanthauzira mchilankhula chomwe woganiziridwa angamve mosavuta. Wina ndiye amanyamula mafailo. Mkango ukazingwa, umadya udzu.
Ku Nkhata Bay, khoti lidagamula Paulos Lungu kukaseweza kundende zaka zitatu atavulaza Julius Mwaluswa kwa Chinguluwe mboma lomwelo.
Bwalolo lidathethetsanso Rute Makuluni, yemwe ali ndi zaka 32, kukaseweza miyezi 6 kundende popezeka ndi chamba.
Wapolisi wofufuza milandu wa pa polisi ya Nkhata Bay, Keston Chiona, adati ganizo la Nyirenda lathandizira kuti musakhale kuthinana kwambiri mzitolokosi zawo.
Chomwe chikuchitika nkuti tikumawatenga oweruza milanduwa kuti akamve milandu. Amene wavomera kulakwa akumupatsiratu chilango. Amene wakana akumupatsa belo kapena kumutumiza kulimande, adatero Chiona.
Naye mneneri wapolisi mchigawo chakumpoto, Peter Kalaya, adati polisi zonse zamchigawocho zimatsata ndondomekoyo.
Timamanga anthu tsiku lililonse kutanthauza kuti zitolokosi zathu nzodzadza. Njira iyi ikuthandiza, adatero Chiona.
Malinga ndi mneneri wa makhoti Mlenga Mvula, ganizoli linadza ngati njira imodzi yochepetsera kuchulukana kwa anthu mzitolokosi za apolisi.
Ndondomekoyi ikuchitika mmaboma onse, adatero Mlenga.
Mneneri wa ndende Smart Maliro adati chiwerengero cha anthu otumizidwa kundende kuchokera kupolisi chidatsika chifukwa anthu amangosungidwa mzitolokosi.
Boma kudzera mwa mlembi wa zachuma Ben Botolo adadzudzula ogwira ntchito mmabwalowa kuti sitalaka yawo ndi yosavomerezedwa ndipo sizitheka kuti boma lipereke ndalama zanyumba zoyambira mchaka cha 2012.
Akutero Botolo: Boma launguza madandaulo anu, koma mfundo ya boma sikusinthasiipereka ndalama zapadera za nyumba.
| 7 |
Gulani mbewu kwa ogulitsa ovomerezekaUnduna Unduna wa malimidwe walangiza alimi kuti ayenera kugula mbewu kuchokera kwa ogulitsa ovomerezeka okha poopa kugulitsidwa mbewu zoonongeka.
Chisale watuluka nkumangidwanso Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Mlembi wamkulu muundunawu, Erica Maganga, wati alimi aike patsogolo mbewu zopezeka msitolo komanso mabungwe amene adalembetsa ku undunawu.
Alimi ayenera kugula mbewu malo ovomerezeka okha Kugulitsa mbewu popanda chilolezo chochoka ku undunawu ndi mlandu waukulu.
Mbewu iyenera kugulitsidwa ndi okhawo ali pa mgwirizano ndi kampani zopanga mbewu.
Ogulitsa mbewu otere amaphunzitsidwa bwino za kagulitsidwe ka mbewuzo komanso kasungidwe kake, adatero Maganga.
Malinga ndi maganga, ogulitsa mbewu ovomerezeka amalandira chiphaso chogulitsira mbewu chomwe chimagwira ntchito kwa chaka chimodzi.
Iye adati onse ofuna kugulitsa mbewu ayenera kulembera kalata ku nthambi yoona za mbewu muundunawu ya Seed Certification and Control Unit.
Ogulitsa amene sakwaniritsa ndondomeko zomwe amapatsidwa pogulitsa mbewu amalandidwa chiphasocho. Cholinga chachikulu nchakuti alimi azigula mbewu zovomerezeka komanso zomwe sizidaonongeke, adatero Maganga.
| 4 |
Mamembala ena a HRDC Atuluka mu Bungwelo Anthu ena omwe akuti ndi okhudzidwa a bungwe la HRDC ati atuluka mu bungweli kamba ka zomwe ati zikuchitika ku bungwelo.
Kudzera pa msonkhano wa atolankhani omwe anthuwa anachititsa lero mu mzinda wa Lilongwe, anthuwa akuti akuona kuti bungwe lomenyera ufululi likulowetsa ndale mu ntchito zake zomwe ati sizoyenera kuti bungwe lowona za maufulu lidzichita.
Mmodzi mwa anthuwa yemwe wati adali msungichuma wa bungweli mboma la Karonga, Chifundo Kapesa wati atsogoleri a bungwe la HRDC akugwiritsa ntchito bungweli pofuna kupeza chikoka cha anthu zomwe wati ndi zosayenera ndipo iye wati mmalo mwake akhala pambuyo pa mgwirizano wa zipani za DPP komanso UDF.
Wati sakuwadziwa anthuwo-Trapence Nkhani yaikulu yomwe tsiku la lero timapereka inali yakuti ife tatuluka mu HRDC chifukwa tawona kuti ku HRDC kuli zolakwika ndipo tinayesetsa kukambirana koma sizinatheke kamba koti bungwelo ndi lomenyera ufulu koma pano silikuchita moteromo, anatero a Kapesa.
Koma wapampando wa bungwe la HRDC Gift Trapence wati ku bungwe lawo kulibe udindo wa msungi chuma ndipo wati ndi odabwa ndi izi.
Ndipo iye wauza Radio Maria Malawi kuti akudziwa kuti anthuwa achita kutumidwa ndi chipani cha DPP kuti ayipitse mbiri ya bungwe lawo ndipo ati awuza maloya awo kuti achitepo kanthu pa nkhaniyi.
| 11 |
Kuphana kwaphweka pa Wenela Tsiku limenelo diraiva wina adati ndikhale kondakitala wa ganyu paulendo wake wolowera ku Machinjiri. Nkhani zinkakamba anthu mmenemo zidali zachilendo kwa ine.
Namwino wina, amene adatsika pa Magalasi ankanena za kachilombo koopsa ka Zika kamene kakuchititsa ana ena a ku Brazil azibadwa ndi mitu yaingono zedi. Nthenda zachilendo zachuluka.
Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Kuchoka apo, namwinoyo ankakamba za mankhwala oopsa otchedwa polonium-210. Ameneyotu ndi poizoni woopsa amene wapha anthu ena otchuka. Asayansi akuti poizoni woopsayu akupezekanso mufodya yemwe ena amakwemba, adapitiriza chiphunzitso namwinoyo.
Abale anzanga, ine nkadatolapo chiyani? Kwa ine kudali kutolera ndalama ndi kutseka chitseko.
Chongoti mayi uja tsikeni, nkhani zidasintha.
Abale, koma tikuphana udyo. Chikuchitika nchiyani? Nkhani ingonongono basi wina wafapo, adatero bambo adakhala mpando wakutsogolo.
Ndi chiyani koma? Ku Machinjiri kwathuku, miyezi iwiri yapitayi nkhanizi ndiye zosayamba. Wantchito wapanja wina paja adapha wantchito wamnyumba nkuthawa ndi matumba atatu a chimanga. Wabizinesi wina wapha wabizinesi mnzake ndipo wina ndi uyu adapezeka ataphedwa nkuchotsedwa maso ndi nkhope. Zoopsa, adayankhira wina.
Si ku Machinjiri kokha. Mwaiwala za bambo wa ku Zingwangwa woombera mkazi ndi mwana wake nkudziphayu? Nanga mwana wa ku Mulanje wapha mayi ake nkuwakwirira mnyumba ati chifukwa amamudzudzula kuba? mtsikana wina amene adavala yunifomu ya sukulu ya za hotela adatero.
Nanga uyu bambo wopha mkazi wake atapeza mauthenga a foni amene amakaikira kuti mkaziyo amatumizira bwenzi lake chonsecho mauthengawo adali a mngono wa mkaziyo yemwe adabwereka foni. Nchiyani chatigwera? adafunsa mkulu wake atanyamula majumbo mosaona zoti ndi pakati pa January.
Mawu anu ali mkamwa, simunamve za mzimayi wapezeka ataphedwa mnyumba yogona alendo ku Bangwe? adafunsa diraiva.
Ndidaikira mangombe: Nanga za mkulu wotuma zigandanga kukapha mkazi wake wakale uja bwanji? Abale anzanga, ndisaname, izi zikundipatsa mantha. Thupi lamera tsemwe. Moyo wa munthu uli mmanja ndithu.
Mungayembekeze zotani mdziko limene mukunena kuti anthu ophwanya malamulo ena asamamangidwe? Poyamba ndimayesatu akadachotsa kaye lamulolo kusiyana ndi kuti ophwanya lamulo asamamangidwe, kapena akamangidwa azitulutsidwa, adatero mkulu wina.
Zoona. Anthutu ogonanana ndi abale awo alipo muno. Tsono akayamba kubwera poyera kuti nawonso alipo ochepa kwambiri ndipo ndi chilengedwe chawo kutero choncho kuwamanga nkuwaphwanyira ufulu. Chipwirikiti chobwera chikhala chotani? adafunsa mzimayi adayandikana naye.
Aliyense mbasimo adangoti duu! Diraiva adatsegula wailesi pomwe aliyense amalingalira za nkhanizo. Padali Moya Pete. Adali maganizo athu kuti Moya Pete akambapo kanthu pa zakuphana chisawawa kukuchitikaku.
Koma ayi.
Yesu anati akakumenyani khofi mbali iyi, mupereke linali. Otsutsa ndi a mabungwe mwandimenya mbali iyi ndakupatsani tsaya linali. Tsono Yesu sadanene kuti mukandimenyanso khofi lina ndichitenji. Mwandimenya katatu tsono ndiona umo ndingachitire, adatero.
Mkulu wina adaseka chikhakhali. Kodi ndimayesa Yesu adati munthu akakulakwira ka 539 uyeneranso kumukhululukiranso ka 539, adatero iye.
| 15 |
Amayi adandaulira boma pa za HIV, edzi Amayi omwe ali ndi kachilombo ka HIV koyambitsa matenda a edzi apempha boma kuti likonze zina mwa mfundo zake zoyendetsera kuti nawonso azitengapo mbali pakayendetsedwe ka ntchito zosiyanasiyana.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Amayiwa apereka miyezi isanu ndi umodzi kuti boma liyankhepo.
Amayiwa analemba chikalata chofotokoza mavuto amene amakumana nawo chifukwa cha malamulo ena ndipo apereka chikalato kwa mkulu wa Nyumba ya Malamulo Henry Chimunthu Banda kuti nyumbayi iunikenso ena mwa malamulo omwe amawaphwanyira ufulu.
Ndikukutsimikizirani kuti mfundo zanu zamveka ndipo kuyambira pa 24 mwezi uno komiti yoyanganira za edzi ndi chakudya chamagulu izikumana kuti iwunike mfundozi ncholinga choti tikamatsegulira zokambirana, mfundozi zidzakhale mgulumo, anatero Chimunthu Banda.
Koma oyanganira za ufulu wa amayi omwe ali ndi kachilombo ka HIV mbungwe la Pan-African Positive Womens Coalition la mmaiko a mu Africa, Tendayi Westerhof, wati boma likuyenera kuchitapo kanthu mmiyezi isanu ndi umodzi ikubwerayi.
Iye wati zikuyenera kukhala choncho chifukwa mavuto amene akukumana nawo amayiwa ndi aakulu kwambiri.
Pokapeleka chikalatacho, amaiwa anapelekezedwa ndi amai anzawo ochokera mmaiko angapo omwe anabwerera msonkhano waukulu oganizira za matenda a edzi pa dziko lapansi.
Mwanfundo zina zomwe ziri mu chikalatacho, amaiwo akuti amamanidwa mwayi wa ngongole zoti angayambire bizinesi kuti azidziyimira paokha. Iwo ati izi zimawachititsa kuti azisowa zoyenerera monga chakudya, makamaka ngati alibe owasamalira.
Chikalatacho chatinso mpaka pano mmadera mwina atsikana amakakamizidwabe kukwatiwa ngakhale mwamunayo asakumudziwa bwinobwino, zomwe akuti zikukweza chiwerengelo cha amayi omwe ali ndi kachilomboka.
Pa mfundo yomaliza mmadandaulo awo, amaiwa apempha boma kuti lisinthe mtundu wa mankhwala otalikitsa moyo a ARV chifukwa omwe alipo tsopanowa amaononga matupi a okumwawo.
Chimunthu Banda anakkhala nawo pa msonkhano waukulu wa maiko osiyanasiyana oganizira za matenda a edzi omwe umachitikira kuno ku Malawi ku Lilongwe.
| 6 |
Zefinati Alick: Kadaulo posema ziboliboli Aluso ndi onse koma luso losema ziboliboli si lachibwana, limafunika khama komanso munthu wolimba mtima. Pa Golomoti mboma la Dedza pali malo otchedwa Golomoti Curios Group amene amapanga ndi kugulitsa ziboliboli. Zefinati Alick nthawi zonse amakhala pamalopa kugulitsa katundu wake uku akupanga wina. BOBBY KABANGO adacheza naye za luso lake motere: Tidziwane wawa Ndine Zefinati Alick, ano ndi malo anga koma zones ndikupangira limodzi ndi mkulu wanga amenenso adandiphunzitsa ntchitoyi.
Alick ndi ziboliboli zake Kodi malo ano adatsekulidwa liti? Adatsekulidwa mu 2012, koma ineyo ndidayamba kusema ziboliboli mu 1998. Panthawiyo ndinkagwirira ntchitoyi ku Mua kenaka ndinkapangira kunyumba kwanga. Mu 2012 mpamene timatsekula malo ano.
Ndi zinthu ziti mumasema? Timasema mtundu ulionse wa zinyama womwe munthu akufuna, chifaniziro cha munthu, Mayi Maria, chifaniziro cha anthu amtundu Wachingoni, galimoto ndi zina zambiri zomwe sindingakwanitse kuzitchula.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Pa Wenela pasintha zedi Mukugwiritsira ntchito mtengo wanji? Pali mitengo yambiri yomwe anthu amagwiritsira ntchito koma ife timakonda mtengo wa mtumbu.
Mumagwiritsira zida ziti popanga katunduyu? Mukakadula mtengowo, mumayenera muyambe kusema ndi sompho, chikwanjenso chimafunika, tchizulo, sandpaper, polishi ndi zida zina ndi zina kuti chomwe tikusemacho chioneke bwino.
Kodi chomwe mwanyamulacho nchiyani? Nanga zimatenga masiku angati kuti ntchito itheke? Mutiuzenso mitengo yake Ichi ndi chifaniziro cha nyama ya chipembere. Chimatenga sabata ziwiri mwina osafikanso malinga ndi nthawi yomwe uli nayo kuti chithe. Chimenechi chikugulitsidwa K10 000. Chinachi ndi chifaniziro cha mayi Wachingoni. Ameneyu amatha mofanana ndi chinyamachi bola ukhale ndi nthawi. Mayiyu timagulitsa K15 000.
Mwathandizika bwanji ndi ntchitoyi? Ndagula nyumba, ndimalipirira ana sukulu komanso feteleza ndimagula kuchokera ntchitoyi. Ndipezereponso mwayi kuwauza anthu kuti ife timapanga chilichonse chomwe akufuna, komanso momwe akufuna chionekere.
| 0 |
Boston Kabango: Chikhomo cha Wanderers Kungomva za Boston Kabango, omwetsa zigoli a matimu ena amayamba kunjenjemera kaamba ka ntchito za mnyamatayu zomwe amazionetsa ku Mighty Be Forward Wanderers komanso ku Flames Under 20. Kodi ntchito zake nzotani? Adayamba bwanji? Nanga tsogolo akuliona bwanji? BOBBY KABANGO akucheza naye motere: Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Mpira si dzitho: Kabango Kodi Boston amamveka uja ndiweyo? Ndine ndithu, musaderere ndi maso okha koma muzipita pabwalo kuona luso lomwe Mulungu adapereka. Dzina langa lonse ndi Boston Bosnho Kabango.
Thupi limeneli umatha kulimbana ndi osewera amatupi awo? Nchifukwa ndikuti musaderere, mpira si kukula thupi koma kukhala ndi mphamvu za mpirawo. Ine ndimayesetsa kuti ndizichita mafizo kuti ndikhale ndi mphamvu zosewerera mpira, osati zoti anthu azindiona nazo.
Kodi udayamba liti kusewera mpira? Luso lidaoneka ndikusewera ku Sporting Leopards mu 2010. Titapita kukapikisana nawo kumpikisano wa Zone 6 anthu adagoma ndi luso langa ndipo Azam Tigers idanditenga. Mu 2015 mpamene ndimabwera ku Nyerere.
Moyo ku Nyerere uli bwanji? Zonse zili bwino, pena tikhumudwe pena kusangalala ndimo moyo umayendera. Kungoti pakati ndidali wovulala ndiye ndatenga nthawi osasewera, pano ndabwereramo.
Uli ndi zaka zingati? Pajatu mumabera zaka anyamata a mpira inu Hahaha! Ayinso osati kubera koma ndili ndi zaka 20.
Maphunziro ndi otani? Nanga uchitanso ziti kupatula mpira? Ndadutsa fomu 4 moti ndikufuna ndipange za umekaniki koma posakhalitsapa ndipitanso kusukulu. Ndimafunitsitsa ntchitoyi kupatula kuti Mulungu adandidalitsa ndi luso la mpira.
Umalota utadzafikira pati? Kukasewera ku England, ilili ndiye loto ndikamasewera mpira.
Ndani amakudolola? Nanga ukafatsa umakonda chiyani? Limbikani Mzava komanso kunja ndi Gary Cahill. Ngati sindikusewera mpira ndiye ndimakonda kuonera makatuni komanso kucheza ndi mayi anga.
| 16 |
Sabuside yayamba ndi njengunje Pulogalamu ya zipangizo za ulimi zotsika mtengo ya sabuside ya chaka chino yayamba koma zokhoma zilipo zambiri kuyerekeza ndi zaka zammbuyomu, nduna ya zamalimidwe Allan Chiyembekeza yavomereza.
Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Polankhula ndi Uchikumbe, Chiyembekeza adati pulogalamuyi yayamba ndi jenkha chonchi kaamba ka mavuto ena monga a zachuma chifukwa boma tsopano likudzidalira palokha pachuma chake.
Ndunayo idati ngakhale ntchitoyi yayamba ndi mavuto oterewa, Amalawi asataye mtima chifukwa boma kudzera muundunawo likudzipereka kuti alimi asavutike.
Anthu kudikira kugula zipangizo zotsika mtengo chaka chatha Tikuvomereza kuti zinthu sizidayambe bwino koma sizikutanthauza kuti zinthu zaipiratu ayi chifukwa padakalipano zipangizo zayamba kale kupita mmadera moti alimi asataye mtima zinthu ziyenda, adatero Chiyembekeza.
Ndunayo idati polingalira mavuto a mayendedwe nthawi ya mvula, ntchitoyi yayamba mmadera ovuta kufikira mdziko lose la Malawi polingalira kuti mvula ikayamba mmadera oterewa galimoto zonyamula zipangizozi zimatitimira kapena kugwa mmatope.
Tayambapo makamaka mmadera ovuta kufikira mvula ikagwa. Panopa madera ambiri oterewa alandira kale zipangizo moti alimi akungodikira makuponi ogulira kuti akagule, adatero Chiyembekeza.
Mkulu wa mgwirizano wa mabungwe a zaulimi wa Civil Society Agriculture Network (Cisanet) Tamani Nkhono Mvula adati boma lachita bwino kubwera poyera nkunena momwe pologalamuyi ikuyendera kuti alimi azidziwiratu zochitika.
Nkhono adati kawirikawiri zinthu zimaonongeka chifukwa chobisa momwe zinthu zilili zomwe zimachititsa kuti alimi azidzidzimutsidwa nthawi yothaitha zinthu zitasokonekera kale.
Pamenepa ife tiyamikire boma chifukwa lapanga zazikulu kubwera poyera. Nthawi zambiri chilungamo ngati ichi chimabisidwa chifukwa cha ndale koma mapeto ake zinthu zimasokonekera,adatero Nkhono.
Iye adati alimi panopa akhale kalikiliki mminda kuyembekeza mvula yobzalira osatengera kuti boma lalankhula bwanji chifukwa iwowo ndiwo amalima osati boma lomwe limangothandizapo.
Alimi ambiri pano ali mminda kukonza kapansi kuti mvula ikangogwa abzale mbewu koma akuti ali ndi nkhawa chifukwa sakudziwa kuti mbewu ndi zipangizo zina ngati feteleza azipeza liti poti sadalandilebe makuponi ogulira.
Amos Dziyende ndi mmodzi mwa alimi omwe adakonza kale munda wake ndipo adati nkhawa yake ili pawiri: Mtengo wa zipangizo ndi nyengo yogulira poti mpaka lero sadalandirebe makuponi ogulira.
Tidakonzeka koma tikumva kuti mtengo wa zipangizo chaka chino wakwera ndiye kaya zitha bwanji komanso mpaka pano makuponi sitidalandire, adatero Dziyende.
Panopa mvula yagunda kale mmadera ena ndipo nthawi iliyonse madzi akhala akugwa pansi kuti dzinja.
| 4 |
Akuti zipolowe zichepe Zipolowe kaamba ka ndale zomwe zakhala zikuchitika mdziko muno zikupereka chiopsezo kuchisankho cha chaka chamawa komanso kutekesa mtendere wa dziko lino, akutero mafumu ndi akwatswiri ena pandale mdziko muno.
Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Iwo atero poona zipolowe zandale zomwe zikuchitika mdziko muno, makamaka kutsatira kumangidwa kwa atsogoleri a zipani zina.
DPP ndi chipani chimene posachedwapa chidaganiziridwa kuti chikukhudzidwa kwambiri ndi zipolowe zamtunduwu. Poyamba, atangomangidwa gavanala wa chipanichi mchigawo cha kummwera, Noel Masangwi ndi ena, otsatirawo adasonkhana kupolisi komwe kumasungidwa anthuwa.
Ndipo atsogoleri a chipanichi, kuphatikizapo mtsogoleri wogwirizira mpando wa pulezidenti, Peter Mutharika, atatengedwa pokhudzidwa ndi nkhani yofuna kutenga boma mwaupandu mtsogoleri wakale wa dziko lino Bingu wa Mutharika atamwalira chaka chatha, otsatira chipanichi adachita zipolowe mmizinda ya Blantrye ndi Lilongwe komanso maboma a Phalombe ndi Thyolo pokwiya ndi kumangidwa kwa atsogoleriwo.
Mkulu wa zakafukufuku mchipanicho, George Chaponda, adauza atolankhani kuti otsatira chipaniwo adachita kutokosoledwa, koma mneneri wa chipanichi, Nicholas Dausi, adanena zotsutsana ndi zomwe adanena Chaponda ponena kuti chipani cha PP ndicho chidapereka makaka a DPP kwa zimbalangondo kuti akachite zipolowezo pofuna kudetsa DPP.
Pounguza izi, Amalawi ena ati ndi bwino otsatira zipani azikhala ndi malire awo chifukwa zotere zikapitirira zingadzabale chisankho choipa mu 2014 komanso mdziko muno mungabuke ziwawa.
Iwo ati ngati wina atadzapambana mokayikitsa ena, zipolowe zotere zingadzachitike ngati Amalawi sathetseratu mchitidwe wosafuna bwalo lamilandu kuti liweruze oganiziridwa kuti ndi opalamula.
T/A Malemia ya mboma la Nsanje wati otsatira zipani akuyenera kudziwa kuti zinthu zikavuta ndi bwino kuzisiya mmanja mwa apolisi komanso ozenga milandu kuti apereke chigamulo.
Monga mfumu yomwe ikusunga anthu azipani zosiyanasiyana, ndine wokhumudwa kwambiri ndi zimenezi, sindikudziwa chifukwa chomwe azipaniwa akuchitira zipolowezi chikhalirecho kuli apolisi ndi mabwalo amilandu. Ili ndi vuto la atsogoleri a zipaniwa chifukwa mwana wanga atapalamula vuto ndikhala ine posamulangiza. Andale akhale pansi ndi azipani awo, adatero Malemia.
T/A Phambala ya ku Ntcheu wati chomwe akufuna ndi mtendere ndipo zipani zichilimike kukhazikitsa mtendere.
Chisankho chikudzachi chikufunika mtendere, kumenyana ayi ndipo izi tonse tikuyenera kuchitapo kanthu, adatero Phambala.
Gulupu Kayiwale ya ku Rumphi yati vuto ndi lakuti ufulu wa demokalase ena adaumvetsa molakwika.
[Kuchita zipolowe] ndi umbuli chifukwa kuli oweruza milandu komanso apolisi, bwanji timachita zotere? Demokalase si imeneyi ndipo tikuyenera kusiya zonse mmanja mwa malamulo kuti agwire ntchito. Andale asabweretse ziwawa ndipo akhale ndi malire awo, adatero Kayiwale.
Mlembi wamkulu ku DPP Dr Allan Chiyembekeza akuti: Sitinakhale pansi kuti tifufuze komanso kukambirana za izi komabe tichitapo kanthu. Mumadziwa kuti pena pake mbale wako atamangidwa zimapwetekabe. Padali zifukwa nchifukwa chake zidachitika zotere, komabe tifufuza.
Naye wachiwiri kwa mneneri wa chipani cha PP Ken Msonda wati chipani chawo chimaonetsetsa kuti chisalowerere nkhani za boma chifukwa woweruza wabwino ndi bwalo lamilandu.
Pachitika zambiri mdziko muno pomwe ife tikulamula koma sitidalowerere chilichonse, mtsogoleri wa dziko lino atalowa mboma adati akufuna kusintha momwe ndale zimachitikira ndipo ichi nchifukwa otsatira chipanichi samapezeka nawo mzisokonezozi, adatero Msonda.
Mneneri wa UDF, Ken Ndanga, wati zipani za mdziko muno zilibe njira zodziwira otsatira chipani chawo. Komabe iye wati chipani chawo chimakhulupirira kuti bwalo ndilo lingapereke gamulo labwino.
Tipemphenso apolisi kuti pogwira ntchito yawo azitsatira malamulo chifukwa ngati izi sizichitika zingameme zipolowe mdziko muno. Zipolowe si zabwino ndipo tonse tidakati tizichita ngati [DPP] pangakhale mpungwepungwe mdziko muno, adatero Ndanga.
Koma kadaulo pa zamalamulo yemwenso ndi mkulu wa bungwe la Justice Link, Justine Dzonzi, wati atsogoleri andale atha kuzengedwa mlandu chifukwa cha zomwe otsatira chipanicho achita ngati patapezeka umboni.
Ngati sipangakhale umboni, ochita zipolowewo atha kuzengedwa mlandu chifukwa chodzetsa chisokonezo, adatero Dzonzi, yemwe adanenetsa kuti zipolowe zotere si zabwino mdziko.
Pa 19 July 2011 otsatira ena a chipani cha DPP adayenda mmizinda ya Blantyre atanyamula zikwanje mmanja ndi kumaopseza kuti athana ndi wina aliyense yemwe achite ziwonetsero zomwe zidachitika pa 20.
Pazisankho za 2004 kudachitikapo ziwawa zitadziwika kuti UDF ndiyo yapambana, pamene anthu ena adali ndi chikhulupiriro kuti adayenera kupambana ndi Mgwirizano Coalition, motsogozedwa ndi Gwanda Chakuamba.
| 11 |
Papa Wapempha Akhritsu Kukhala Okhazikika pa Chikhulupiliro Chawo Mtsogoleri wa mpingo wa katolika pa dziko lonse Papa Francisco wati akhristu akuyenera kukhala anthu osagwedezeka pa chikhulupiriro chawo.
Papa Francisko Papa Francisco walankhula izi loweruka pa Misa yomwe anatsogolera ku likulu la mpingowu ku Vatican.
Iye wati ngakhale apostoli adakumana ndi mavuto osiyana-siyana pofalitsa uthenga wa chipulumutso, sadalore kuti mavutowo achepetse kapena kuthetseratu chikhulupiriro chawo mwa Mulungu koma mmalo mwake adali olimba mtima komanso a chikhulupiriro.
Pamenepa Papa Francisco wati akhristu akuyenera kutengera chitsanzo pokhala olimba mtima, osagwedezeka ndipo a chikhulupiliro pofalitsa uthenga wa chipulumutso.
| 13 |
Ziwawa pa Ndale ndi Kubera Chisankho-Chilima Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino yemwenso ndi mtsogoleri wa chipani cha UTM, Dr. Saulos Klaus Chilima wadzudzula mchitidwe wa ziwawa pa ndale ponena kuti kutero ndi kubera chisankho.
Dr. Chilima wanena izi pa msonkhano wa atolankhani womwe chipanichi chinachititsa mu mzinda wa Lilongwe kutsatira ziwawa pa ndale zomwe anthu ena omwe akuganiziridwa kuti ndi a chipani cholamula cha Democratic Progressive (DPP) akhala akuchitira zipani zotsutsa boma mdziko muno. Iye wati kuwopsezana pa ndale kumachititsa kuti anthu ena alephere kuchita kampeni komanso kuvota momasuka zomwe wati ndi njira imodzi yobera chisankho.
Dr. Chilima wadzudzula mtsogoeri wa dziko lino poyanganira mchitidwe wa ziwawa mdziko muno ndipo wamupempha kuti achitepo kanthu msanga.
| 11 |
Mudali mu Sitandede 1 Dzina la Julius Mithi si lachilendo. Ndi kadaulo pa zowerengetsa komanso wagwirapo ntchito kubungwe la zamasewero la FAM. Ngakhale ambiri angamudziwe mkuluyu, zambiri za banja lake sizidziwika komanso momwe adatumbira namwali wake.
Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Mithi akuti naye ndi wosongoka pakamwa ndipo adatumba kale womusangalatsa. Uyu ndi Ella Msopa Kumwenda amene lero ndi mayi Mithi.
Mithi ndi mkazi wake Ella Ndi banja lachitsanzo, lonyadirana ndipo Mulungu sadalimane mphatso za ana awiri kuwonjezera chimwemwe chawo. Kodi nanga Mithi adamasuka bwanji pakamwa kuti athere mawu Ella? Chithokozo chipite kwa makolo a awiriwa potumiza ana awo ku Vongo FP School mboma Mzimba. Awiriwatu adaponyerana maso ali sitandede 1.
Kodi nthawi imeneyi Mithi adali atadziwa kale kusula Chichewa? Ayi, timangokondana mwachibwana.
Nanga Chichewa adasula pati? Ndinachoka ku Vongo kubwera ku Mzuzu mu 1981 kudzakhala ndi bambo anga ndipo panadutsa zaka 7 pomwe sitinathe kuonana, kufikira ine nditayamba ntchito mboma mu 1992. Apo Ella anali ku Ekwendeni Nursing School. Mwamwawi tinadzakumana ku Mzuzu pomwe chibwenzi chathu chidayambiranso. Atatha zaka 4 kusukulu ya unamwinoko tidakwatirana.
Mithi akuti zinthu izi zidamukoka kuti asadumphitse mawu pa wokondedwa wakeyu: Ndinamufunsira chifukwa adali mtsikana wofatsa komanso amachoka kwathu, kwawo ndi kwa agogo anga.
Okondanawa akuti panthawiyo adalibe ndalama zomangitsira ukwati ndipo adangodalitsa ku St Peters Cathedral Parish ku Mzuzu mu 2008.
| 3 |
Kupewa nsabwe za mfodya ndi pano Nsabwe za mufodya ndi gwero limodzi lomwe limachititsa kuti fodya avute malonda kumsika ndipo vutoli likagwera mlimi, chaka chimenecho amalirira kuutsi kaamba koti ngati ogula sadagule fodyayo pamitengo yolira ndiye kuti wabwezedwa.
Malingana ndi katswiri wa zafodya, vutoli ndi lopeweka ndipo kapewedwe kake nkosabowola mthumba poyerekeza ndi zomwe zimalowa pofuna kupulumutsa fodya nsabwezo zikalowa.
Chakwera akwanitse malonjezoHRDC Masankhidwe a nduna autsa mapiri pa chigwa Malonjezo ayamba kuoneka Mkulu wa bungwe la alimi a fodya la Tobacco Association of Malawi (Tama), Reuben Maigwa, wauza Uchikumbe kuti vuto lalikulu la nsabwe za mufodya ndi lakuti zimateketa fodya nkukhala ngati wagayidwa kale ndiye ukapita kumsika, ogula sachita naye chidwi.
Ogula fodya amayangana mtundu, makulidwe ndi kukhuthala kwa masamba a fodya, osati ufa wa fodya, ayi. Ndiye amati akatsegula belo nkuonamo ufa amaona ngati ndi fodya wachinyengo ndipo amamubweza. Zikatero ndiye kuti chaka chimenecho zadapo, adatero Maigwa.
Iye adati nthawi yopewa vuto la nsabwe za mufodya ndi ino poti ikayambika ntchito yothyola fodya mpata umasowa komanso zimathandiza kuti nsabwezo zisakhale ndi mpata wokwanira oswana.
Mkuluyu adati nthawi zambiri gwero la nsabwezi limakhala zipangizo zomwe zidagwiritsidwa ntchito chaka chinzakecho zomwe zidakhudzidwa ndi nsabwe kapena malo osungiramo fodya panthawi yoyembekezera kupita kumsika.
Tikunena pano, alimi ena adayamba kale kusonkhanitsa zipangizo ngati ziguduli zodindira mabelo, ulusi wosokera ndi zipangizo zina ndipo zimenezi ndizo zimatha kuyambitsa nsabwe ngati komwe zidagwira ntchito mmbuyomo kudali vuto la nsabwe.
Kupewa kwake nkosavuta chifukwa choyenera nkuchapa zipangizo zoterezi bwinobwino nkupopera mankhwala usadasunge pamalo abwino kudikira ntchito yake, adatero Maigwa.
Iye adati kuchapa ndi kupopera kokha sikukwanira ngati malo osungiramowo sali osamalika chifukwa nsabwezo nthawi zina zimatsakamira mmakoma ndiye ngakhale zipangizo zitasamalidwa bwino nkusungidwa mmalo omwe muli nsabwe palibe chomwe chachitika.
Chaka chilichonse malonda a fodya akatha timayenera kutsuka makoma onse a momwe timasungiramo fodya wathu ndi pansi pomwe nkupoperamo makhwala kuti tizilombo ngati nsabwe tife, adatero Maigwa.
Iye adati alimi ambiri amagwa mmavuto ndi nsabwe za fodya kaamba kolekerera nkumaganiza kuti nthawi idakalipo kenako akaona kuti zawakoka manja amayamba kuchita zachidule ntchito nkumaonongeka.
Fodyatu sachedwa, posachedwapa ena ayamba kuthyola ndiye ikangofika nthawi imeneyi mpata umasoweratu chifukwa umati mmawa uli kothyola, masana ukusoka uku ukupachika mmikangala ndiye zoti ungapeze mpata wokachapa ziguduli kapena kukakonza mosungira mpovuta, adatero katswiriyu.
Maigwa adatiso nthawi yomwe ino ndiye yofunika kuyambapo kukonza zigafa ngati zidaonongeka kapena ngati palibiretu kuti pomwe fodya azidzachoka kumunda kubwera kumudzi adzakhale ndi pofikira, osati zomwe amachita ena zopachika fodya mkhitchini mophikira chifukwa chosowa malo osungiramo fodya.
| 4 |
Adona Hilida akadangobwera Ngakhale pa Wenela padali zovuta, malo aja timakonda padali kuphulika nyimbo.
Ine nilibe pulobulemu Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Nilibe pulobulemu.
Chifukwatu timayembekezera kuti wotisiyayo mtembo wake ufika masana a tsiku limenelo.
Titakhala pamalopo, adabwera mkulu wina akuthamanga.
Akuluakulu,tiyeni mukandithandize kukhazikitsa mtima pansi bambo a malemu, akufika kumene kuchokera kwawo kwa Govala, adatero mkulu uja, thukuta lochita kusamba.
Tidakhamukira komweko! Koma mkulu adavuta.
Mwana wanga Boyisi waferanji? Boyisi anditumizira bulangete kuchoka ku Joni ndani? Ndikuti osandigwira! adali kulira mkuluyo.
Pepani, pepani, wina ankayesera kumutonthoza.
Mkulu adali ndi mavuvu! Osandigwira! Boyisi waferanji mwana wanga? Bwanji sunandifonere kuti unditsanzike? Osandigwira ineeeeee! Anthu okwana 10 adakwanitsa kumukhazika pansi. Adali kufwenthera ndipo ine ndidakhala moyandikana naye.
Mwamwa kale tiyi? adandinongoneza mkuluyo.
Abale anzanga, matchona amayenera kubwera kumudzi akakhalakhala kunjako.
Nkhani idayala nthenje pa Wenela usiku umenewo kusiwa idali ya matchona.
Koma mtchona wamkulu ndi Adona Hilida! Makhrisimasi awiri ndithu ali mliyenda! Ndalama ali nazo, adatero Gervazzio.
Ali ku exile! Anyamata ambiri amakhala ku exile asanalande ulamuliro koma Adona Hilida adathawira kunja ulamuliro utawasempha, ntchito za manja awo poboola mipopi ya chuma zitawachitira umboni, adatero Abiti Patuma.
Muli ndi umboni wanji kuti zikuwakhudza? Mudaliko? adafunsa mkulu amene adali naye tsiku limenelo.
Mufunanso umboni wotani kuposa zomwe zikuonekeratuzi? Adathawiranji? Nanga anthu onse akuwatchula Adona Hilidawa angakhale kuti akulota? adayankha Abiti Patuma.
Abale anzanga, inetu zimandisempha.
Ndipo akadangobwera nthawi ya Khrisimasiyi chifukwatu ndiye chochita sangachisowe. Akhoza kumagulitsa nawo mabaluni ngakhalenso makombola awandawa. Chochita sichingasowe, adatero Gervazzio.
Komanso anthu onsewa akuti ndalamazo zidali zakuti Polisi Palibe idzaluzire mpando wonona. Onsewa ngamisala? Akuopa chiyani Adona Hilida? Akadangobwera kuti mlandu wa munda tidzaukambire pamunda pawo pomwepo, adatero Abiti Patuma.
Kwa ine, ndingothokoza kuti sindili mtchona ngati Adona Hilida. Ndimapuma mpweya mopanda kucheuka! Kusankha nkwanga kuti ndisangalale Khrisimasi kapena ayi. Pajatu kwathu kwa Kanduku timakhulupirira kuti chisangalalo cha Khrisimasi chidalipo kuyambira kale, Yesu asadabadwe.
Koma izotu sindizitengera kwenikweni pozindikira kuti uzimu ndiwo ufunika.
Sindikulalikira, koma ndi bwino kuthokoza kuti taonanso Khrisimasi ina! Ndi bwino kumayamika Mulungu chifukwa mwamwayi nkutsetserekera mu 2016. Zaka ndiye zikukhamukira ku 2019 kuti tidzaone Adona Hilida ndi Polisi Palibe akuthotha Moya Pete ndi Dizilo Petulo Palibe.
| 15 |
Anatchereza Amandimenya Anatchereza, Chisale watuluka nkumangidwanso Sipakala waimitsa Nyumba ya Malamulo Pa Wenela pasintha zedi Ndine mtsikana wa zaka 19 ndipo ndili ndi bwenzi la zaka 21 yemwe ndili naye mwana mmodzi. Dandaulo langa ndi loti akandipeza ndikucheza ndi anyamata amandimenya ngakhale kuti sitinakwatirane. Koma iyeyo amachezanso ndi atsikana ena koma ine sindiyankhulapo kanthu. Nthawi ina adandimenya mpaka kukomoka. Nditani agogo anga? LWT, Chilobwe, Blantyre LWT, Ndamva vuto lako, mwana wanga. Kuchitirana nkhanza mbanja kaya pachibwenzi si chinthu chololedwa ngakhale pangono ndipo aliyense wochitira mnzake nkhanza zamtundu uliwonse akulakwira malamulo ndipo atasumiridwa ayenera kulangidwa ameneyo. Zimatheka bwanji kuti anthu okondana azichitirananso nkhanza pomenyana? Wachita bwino kubweretsa vuto lako poyera chifukwa alipo ena amene akumachitiridwa nkhanza ndi okondeka awo koma zimangothera mmimba, ati kumenyana ndi mankhwala a banja. Si zoona zimenezi. Tsono iwe utamenyedwa ndi bwenzi lakolo mpaka kukomoka basi udangokhala duu! Nawenso ndiye kuti ndi wopepera! Adzakuphatu ameneyo ukapanda kusamala naye. Zikadzachitikanso uyenera kukamuneneza kupolisi kapena kumabungwe amene amayanganira za maufulu a anthu kuti adzakuthandize chifukwa akukuphwanyira ufulu wako ameneyo. Nditengerepo mwayi wolangiza achinyamata kuti kukhala ndi ana musadalowe mbanja zotsatira zake zimakhala ngati zimenezi. Chibwana basi! Zichepe chonde.
Ndikumukondabe Zikomo Anatchereza, Ndine bambo wa zaka 30 ndipo ndili ndi ana awiri. Vuto lomwe ndili nalo ndi loti mkazi ndinabereka naye ana anandithawa miyezi 11 yapitayo ati ndimamuvutitsa. Pakalipano ndapeza mkazi wa zaka 20 ndipo akunetsa kuti amandikonda. Ndinamuuza chilungamo chonse chokhudzana ndi ana ndipo adamvetsa. Ndithandizeni maganizo poti wakaleyo ndimamukondabe limodzi ndi ana anga. Koma wapanopayunso ali ndi pathupi panga. Ndithandizeni chonde.
ZTB ZTB, Nkhani yanu ndi yovuta ndipo sindidziwa kuti ndikuthandizani bwanji. Choyamba mwanena kuti mkazi wanu woyamba amene muli naye ana awiri adakuthawani chifukwa ati ndinu wovuta. Kuvuta kwake kotani? Inu mukuti mumamukondabe ndi ana, koma pano mulinso pachibwenzi ndi mayi wa zaka 20, yemwe pano ndo woyembekezera. Mafunso nawa: Ngati mkazi adakuthawaniyo mumamukondadi, mudachitaponji kuti mubwererane? Ngati mumamukondadi, chidachitika nchiyani kuti mugwenso mchikondi ndi mtsikana wa zaka 20 mpakana kumupatsa pathupi musanamukwatire? Chimene ndikuona apa ndi chinyengo kumbali yanu ndipo ndinu wovutadi abambo inu. Ndinu wachimasomaso ntheradi! Poti munthu sudziloza chala, mwina mkazi wanu woyambayo adaona kuti ndinu wovuta ndi nkhani yokonda akazi koma muli pabanja. Tsono ngakhale mutabwererana ndi mkazi adathawayo, nanga mwana wa eni mwamutupitsa mchomboyo mumutani? Zofunatu izo! Mukuvutitsa ana osalakwa, za zii! Ndikufuna bambo anga Anatchereza, Ndine Efrida Lungu kwa Kayembe, T/A Wimbe ku Kasungu. Ndimangomva kuti bamboo anga ndi a Lungu, Achitumbuka ndipo akuti alipo. Ine ndimafunitsitsa nditawaona. Akuti ankaphunzitsa pa Chamama School ndi pa Chimbowe. Akuti adandisiya ndili ndi zaka ziwiri koma pano ndili ndi zaka 19 ndipo ndili Form 4. Amene angawadziwe chonde tilumikizane pa 0999 810 665/0885 831 843/0997 249 347 . Ambuye akudalitseni.
Ofuna banja Ndine mayi wa zaka 26 ndikufuna mwamuna wa zaka 28. Ndili ndi mwana mmodzi. Mwamunayo akhale Mkatolika. Wondifuna aimbe pa 0884 484 963.
| 12 |
CSEC Yapempa University za Malawi Ziyambe Kugwira Ntchito Pazokha Bungwe lomenyera ufulu wa maphunziro mdziko muno la Civil Society For Education Coalition Network lati kuchedwa kwa sukulu za ukachenjede zomwe anazichotsa mu University ya Malawi kuti ziyambe kugwira ntchito kukusokoneza maphunziro mdziko muno.
Mkulu wa bungweli a Benedicto Kondowe ndi omwe anena izi polankhula ndi Radio Maria Malawi.
Iwo ati ndi zokhumudwitsa kuti boma silinasankhebe akuluakulu oyendetsa sukuluzi (Vice Chancellor) zomwe ati zikukhudza kaperekedwe ka maphunziro msukuluzi.
Tikudikira gawo lotsiriza pa ndondomekoyi-Gama Koma polankhulapo wapampando wa University ya Malawi, mbusa Dr. Billy Gama wati pakadali pano akudikira gawo lotsilizira kuti ma University amenewa akhale oyima pawokha ndi kuyamba kugwira ntchito zawo.
Tikudikirabe gawo lotsiriza la zokonzekerazi lomwe limatchedwa kuti commitment notice kaamba koti ndi yomwe inapatsidwa mphanvu kupereka ku ministry of education kuti tsopano ma college aja akonzeka bwinobwino ndipo akhonza kuyima pawokha, anatero Dr. Gama.
Mwazina iwo ati akufuna kuti akazagawa ma university wa adzakhale kuti akonzeka kuziyimira pawokha komanso kunja kwa dziko lino choncho akuyenera kuchita zinthu mu dongosolo lake kuti zikhale zapamwamba.
| 3 |
Akhutira ndi mitsutso ya atsogoleri andale Akatswiri andale akhutira ndi mitsutso ya atsogoleri omwe akudzaima nawo pa zisankho zapatatu zomwe zichitike mdziko muno pa May 21 chaka chino.
Akatswiriwa ati mitsutsoyi ndi yofunika kwambiri pa ndale za demokalase kaamba koti imapereka mwayi kwa atsogoleri wotambasula mfundo zawo za chitukuko.
Pa Wenela pasintha zedi ANatchereza Tidakumana ku sukulu ku Chiradzulu Mary Chilima, ndi phungu wa kummwera kwa boma la Mzimba, Agness Nyalonje, kucheza ku mtsutso wa atsogoleri ku Lilongwe Iwo adati chokondweretsa nchoti anthu akupatsidwa mwayi wofunsa pamene sakumvetsetsa.
Mmodzi mwa akatswiriwa, Rafiq Hajat, adati mmbuyomu atsogoleri samakhala ndi mwayi wotambasula mfundo zawo kwa anthu omwe akufuna kuti adzawavotere.
Ndikadakondwa mfundo zomwe atsogoleriwa akutulutsa zikadalembedwa ndi kusayinira kuti mtsogolo asadzakane akadzafunsidwa, adatero Hajat.
Iye adapempha omwe akuyendetsa mitsutsoyo kuti azipereka nthawi yokwanira yoti anthu azifunsa atsogoleriwo.
Ngakhale anthu ambiri amasankha atsogoleri potengera zipani komanso zigawo zomwe amachokera, kadaulo wa ndale wa ku Chancellor College, Mustafa Hussein, adasindika kufunika kwa mitsutso.
Anthu ena amasankha atsogoleri potengera mfundo zomwe akutulutsa. Pachifukwa ichi, tiyeni tipititse patsogolo mitsutso ya atsogoleri, adatero Hussein.
Koma kadauloyu adapempha omwe akuchititsa mitsutsoyo kuti samakondere mtsogoleri wina aliyense.
Ngakhale akatswiriwa akuti mitsutsi ikupindula, mfumu Mkumpha ya mboma la Likoma ikuti palibe chaphindu chomwe ikuonapo.
Atsogoleriwa akungotinamiza, akadzalowa mboma sadzapanga zomwe akuuza anthu lero.
Ndikadakhala ndi nambala zawo ndikadawaimbira nkuwauza kuti asatimate phula mmaso, adatero Mkumpha.
Godfrey Masawo akugwirizana ndi maganizo a mfumuyi.
Pothirirapo ndemanga patsamba la mchezo la Facebook la kampani yosindikiza nyuzipepala ya Nation Publications Limited (NPL), Masawo adati: Zinazi ndi mkambakamwa chabe atsogoleriwa sadzakwanitsa.
Koma alembi a zipani za ndale akuti ndi wokhutira ndi momwe mitsutsoyi ikuyendera.
Mlembi wa UTM, Patricia Kaliati, ndi wa Malawi Congress Party (MCP), Eisenhower Mkaka, adati zipani zawo zikudzigulitsa mokwanira kudzera mmitsutsoyo.
Tithokoze mabungwe omwe akonza mitsutsoyi chifukwa yatithandiza kuti tizigulitse kwa anthu ambiri.
Ndikudziwa kuti mitsutsoyi iwonjezera mavoti omwe tipeze, adatero Kaliati.
Komanso kafukufuku akuonetsa kuti anthu ambiri akutsatira mitsutsoyo pa masamba a michezo monga Facebook, Twitter ndi WhatsApp.
Mwachitsanzo, anthu 6 700 ndiwo amatsatira mtsutso wa atsogoleri a zipani za ndale womwe udachitika pa March 29 ku Bingu International Conference Centre (Bicc) mu mzinda wa Lilongwe.
Pamene anthu okwana 2 200 adaonera mtsutso wa otsatira kwa atsogoleri a zipani womwe udachitika pa March 26 mu mzinda wa Mzuzu.
| 11 |
Subsets and Splits